LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb16 March tsa. 1
  • Maulaliki Acitsanzo

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Maulaliki Acitsanzo
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Tumitu
  • Nkhani Zofanana
  • NSANJA YA MLONDA
  • NSANJA YA MLONDA (tsamba lothela)
  • KAPEPALA KOITANILA ANTHU KU CIKUMBUTSO
  • LEMBANI ULALIKI WANU
  • Maulaliki a Citsanzo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Maulaliki Acitsanzo
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Maulaliki a Citsanzo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Maulaliki Acitsanzo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
mwb16 March tsa. 1
Akucita Cikumbutso ca imfa ya Kristu

Akucita Cikumbutso ca Imfa ya Kristu ku Germany

Maulaliki Acitsanzo

NSANJA YA MLONDA

Magazini a Nsanja ya Mlonda, Na. 2 2016 | N’cifukwa Ciani Yesu Anavutika ndi Kutifela?

Funso: Kodi mau odziŵika bwino awa mumawamvetsetsa?

Lemba: Yoh. 3:16

Kugaŵila Cofalitsa: Nsanja ya Mlonda iyi, ifotokoza mapindu amene mungapeza cifukwa cakuti Yesu anavutika ndi kutifela.

NSANJA YA MLONDA (tsamba lothela)

Funso: Onani funso ili ndi mayankho amene anthu ambili apeleka. [Ŵelengani funso loyamba ndi mayankho ake.] Kodi inu mungayankhe bwanji?

Lemba: Mat. 4:1-4

Kugaŵila Cofalitsa: Popeza Mdyelekezi anakamba ndi Yesu ndi kumuyesa, ndiye kuti Mdyelekezi alikodi osati kuti ndi maganizo oipa cabe. Kodi Baibulo limakamba ciani za Mdyelekezi? Magazini iyi ikufotokoza zambili.

KAPEPALA KOITANILA ANTHU KU CIKUMBUTSO

Kapepala Koitanila Anthu ku Cikumbutso ca imfa ya Kristu mu 2016

Kugaŵila Kapepala: Tikupatsa anthu tumapepala towaitanila ku mwambo wofunika kwambili. [Patsani mwininyumba kapepala.] Pa March 23, anthu mamiliyoni padziko lonse lapansi adzasonkhana kuti akumbukile imfa ya Yesu Kristu, ndi kumvetsela ku nkhani ya m’Baibulo yaulele imene idzafotokoza mapindu amene tidzapeza cifukwa ca imfa yake. Pa kapepala aka alembapo malo ndi nthawi kumene kudzacitikila mwambo umenewu kuno kwathu. Conde mukabwele.”

LEMBANI ULALIKI WANU

Onani maulaliki acitsanzo amene asonyezedwa kale kuti akuthandizeni kulemba ulaliki wanu.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani