LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 April tsa. 4
  • “Macimo Ako Akhululukidwa”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Macimo Ako Akhululukidwa”
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Nkhani Zofanana
  • Yehova Adzakucilikizani
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Yesu Acita Cozizwitsa Cake Coyamba
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • “Mukhale Oyela”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Yehova Analenga Zamoyo pa Dziko Lapansi
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 April tsa. 4
Yesu ali pa mpando wake wacifumu kumwamba

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | MALIKO 1-2

“Macimo Ako Akhululukidwa”

2:5-12

Munthu wakufa ziwalo akutsitsidwila kwa Yesu kupitila pa m’boo wa pa denga

Tiphunzilapo ciani pa cozizwitsa ici?

  • Kudwala kunabwela kaamba ka ucimo

  • Yesu ali na mphamvu zokhululukila macimo na kucilitsa odwala

  • Mu Ufumu wa Mulungu, Yesu adzacotsa ucimo na matenda kwamuyaya

Kodi lemba la Maliko 2:5-12 linganithandize bwanji kupilila nikadwala?

Munthu wosaona wayamba kuona; munthu wolemala wasiya kalikisho na kuyamba kuyenda
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani