Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Mlaliki 2:4-8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ndinagwira ntchito zikuluzikulu.+ Ndinamanga nyumba zambirimbiri.+ Ndinalima minda ya mpesa yambirimbiri.+ 5 Ndinakonza minda yokongola komanso malo odzalamo maluwa ndi mitengo. Ndipo ndinadzalamo mitengo ya zipatso zosiyanasiyana. 6 Ndinapanga madamu a madzi kuti ndizithirira mitengo imene inamera mʼnkhalango yanga. 7 Ndinali ndi antchito aamuna ndi aakazi+ komanso ndinali ndi antchito amene anabadwira mʼnyumba mwanga.* Ndinalinso ndi ziweto zochuluka zedi, ngʼombe ndi nkhosa.+ Zinali zambiri kuposa za onse amene anakhalapo mu Yerusalemu ine ndisanakhalepo. 8 Ndinapeza siliva ndi golide wambiri,+ chuma chimene mafumu amakhala nacho* ndiponso chimene chimapezeka mʼzigawo za dziko.+ Ndinali ndi oimba aamuna ndi aakazi. Ndinalinso ndi akazi ambiri, omwe amasangalatsa kwambiri mtima wa amuna.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani