Numeri 9:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 “Tsopano ana a Isiraeli akonze nsembe ya pasika+ pa nthawi yake yoikidwiratu.+ Yoswa 5:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Ana a Isiraeliwo anakhalabe ku Giligala. Anachita pasika madzulo pa tsiku la 14 la mweziwo,+ ali m’chipululu cha Yeriko. 2 Mafumu 23:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Tsopano mfumuyo inalamula anthu onse kuti: “Chitirani pasika+ Yehova Mulungu wanu, malinga ndi zimene zalembedwa m’buku la panganoli.”+ 2 Mbiri 35:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Muphe nyama ya pasika+ n’kudziyeretsa+ ndipo muikonzere abale anu kuti muchite mogwirizana ndi mawu a Yehova kudzera mwa Mose.”+ Ezara 6:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Chifukwa chakuti ansembe ndi Alevi anadziyeretsa+ monga gulu limodzi, onse anali oyera. Choncho Aleviwo anapha nyama ya pasika+ ya anthu onse amene anachokera ku ukapolo, ya abale awo ansembe, ndiponso yawo. Luka 22:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Tsopano tsiku la chikondwerero cha mikate yopanda chofufumitsa linafika, tsiku loyenera kupha nyama yoperekera nsembe ya pasika.+
10 Ana a Isiraeliwo anakhalabe ku Giligala. Anachita pasika madzulo pa tsiku la 14 la mweziwo,+ ali m’chipululu cha Yeriko.
21 Tsopano mfumuyo inalamula anthu onse kuti: “Chitirani pasika+ Yehova Mulungu wanu, malinga ndi zimene zalembedwa m’buku la panganoli.”+
6 Muphe nyama ya pasika+ n’kudziyeretsa+ ndipo muikonzere abale anu kuti muchite mogwirizana ndi mawu a Yehova kudzera mwa Mose.”+
20 Chifukwa chakuti ansembe ndi Alevi anadziyeretsa+ monga gulu limodzi, onse anali oyera. Choncho Aleviwo anapha nyama ya pasika+ ya anthu onse amene anachokera ku ukapolo, ya abale awo ansembe, ndiponso yawo.
7 Tsopano tsiku la chikondwerero cha mikate yopanda chofufumitsa linafika, tsiku loyenera kupha nyama yoperekera nsembe ya pasika.+