Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 8:56
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 56 “Adalitsike Yehova+ amene wapatsa anthu ake Aisiraeli malo ampumulo, monga mwa zonse zimene analonjeza.+ Palibe mawu ndi amodzi omwe+ amene sanakwaniritsidwe pa malonjezo ake onse abwino amene analonjeza kudzera mwa Mose mtumiki wake.+

  • 1 Mbiri 23:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Davide anachita zimenezi popeza anati: “Yehova Mulungu wa Isiraeli wapereka mpumulo kwa anthu ake,+ ndipo iye adzakhala mu Yerusalemu mpaka kalekale.+

  • Aheberi 4:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Pakuti ngati Yoswa+ anawalowetsa m’malo ampumulo,+ Mulungu sakananenanso pambuyo pake+ za tsiku lina.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena