Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 4:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Koma nonsenu amene mukumamatira+ kwa Yehova Mulungu wanu muli ndi moyo lero.

  • Deuteronomo 10:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 “Muziopa Yehova Mulungu wanu.+ Muzim’tumikira,+ kum’mamatira+ ndi kulumbira pa dzina lake.+

  • Rute 2:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Yehova akudalitse chifukwa cha zimene wachita,+ ndipo Yehova, Mulungu wa Isiraeli akufupe mokwanira.+ Iye amene m’mapiko mwake wathawiramo ndi kupezamo chitetezo.”+

  • 1 Mafumu 8:41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 “Komanso mlendo+ amene sali mmodzi wa anthu anu Aisiraeli, amene wabwera kuchokera kudziko lakutali chifukwa cha dzina lanu+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena