Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 27:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Musankhe munthu woti akhale mtsogoleri wawo pa zinthu zonse, woti aziwatsogolera pa zochita zawo zonse,+ kuti khamu la Yehova lisakhale ngati nkhosa zopanda m’busa.”+

  • Deuteronomo 28:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 “Udzadalitsika pa zochita zako zonse.+

  • 1 Samueli 29:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Choncho Akisi+ anaitana Davide ndi kumuuza kuti: “Pali Yehova, Mulungu wamoyo,+ iweyo ndiwe wowongoka mtima, ndipo ndasangalala+ kuti wabwera nane+ kunkhondo, pakuti sindinapeze choipa chilichonse mwa iwe kuyambira tsiku limene unabwera kwa ine kufikira lero.+ Koma olamulira ogwirizana+ sakukuona bwino.

  • Salimo 121:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Yehova adzakuteteza pa zochita zako zonse,+

      Kuyambira tsopano mpaka kalekale.+

  • Yesaya 37:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Ukakhala phee, ukamatuluka,+ ndiponso ukamalowa, ine ndimadziwa bwino,+

      Ndimadziwanso ukandipsera mtima,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena