2 Samueli 8:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Davide anakhazikitsa midzi ya asilikali mu Edomu.+ Mu Edomu yense anaikamo midzi ya asilikali, moti Aedomu anakhala antchito a Davide+ ndipo Yehova anali kupulumutsa Davide kulikonse kumene anali kupita.+ 1 Mafumu 22:47 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 47 Pa nthawi imeneyo ku Edomu+ kunalibe mfumu. Nduna ndi imene inali kulamulira monga mfumu.+ Mlaliki 4:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Ngati wina angagonjetse munthu mmodzi, anthu awiri akhoza kulimbana naye.+ Ndipo chingwe chopotedwa ndi zingwe zitatu sichingaduke msanga.
14 Davide anakhazikitsa midzi ya asilikali mu Edomu.+ Mu Edomu yense anaikamo midzi ya asilikali, moti Aedomu anakhala antchito a Davide+ ndipo Yehova anali kupulumutsa Davide kulikonse kumene anali kupita.+
12 Ngati wina angagonjetse munthu mmodzi, anthu awiri akhoza kulimbana naye.+ Ndipo chingwe chopotedwa ndi zingwe zitatu sichingaduke msanga.