Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 58:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Woipayo amayenda ngati nkhono imene ikusungunuka.

      Iwo sadzaona dzuwa ngati mwana wa mayi amene wapita padera.+

  • Mlaliki 6:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ngati munthu atabereka ana 100+ n’kukhala ndi moyo zaka zambirimbiri, masiku a moyo wake n’kukhala ochuluka,+ koma moyo wake osakhutira ndi zinthu zabwino,+ komanso osalowa m’manda,+ ndithu mwana amene anabadwa wakufa ali bwino kuposa iyeyu.+

  • Hoseya 9:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Inu Yehova, apatseni zimene mukuyenera kuwapatsa.+ Chititsani kuti mimba zawo zizipita padera+ ndiponso mabere awo afote.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena