Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 47:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Pakuti Yehova, Wam’mwambamwamba, ndi wochititsa mantha,+

      Ndiye Mfumu yaikulu padziko lonse lapansi.+

  • Salimo 145:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ufumu wanu ndi ufumu umene udzakhalapobe mpaka kalekale.+

      Ulamuliro wanu udzakhalapobe ku mibadwo yonse.+

  • Yesaya 14:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Izi ndi zimene ndatsimikiza kuchitira dziko lonse lapansi, ndipo ili ndi dzanja limene latambasuka kuti likanthe mitundu yonse ya anthu.

  • Danieli 4:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Inuyo adzakuthamangitsani pakati pa anthu ndipo muzidzakhala pakati pa nyama zakutchire.+ Muzidzadya udzu ngati ng’ombe+ ndipo muzidzanyowa ndi mame akumwamba. Ndiyeno padzadutsa nthawi zokwanira 7+ kufikira mutadziwa kuti Wam’mwambamwamba ndiye Wolamulira wa maufumu a anthu,+ ndiponso kuti akafuna kupereka ulamuliro kwa munthu aliyense, amamupatsa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena