Rute 4:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Pamenepo anthu onse ndi akulu amene anali pachipata anayankha kuti: “Ndife mboni! Yehova adalitse mkazi amene akulowa m’nyumba mwako kuti akhale ngati Rakele+ ndi Leya,+ akazi amene anabereka ana a nyumba ya Isiraeli.+ Uonetse kulemekezeka kwako mu Efurata+ ndi kudzipangira dzina m’Betelehemu.+ 1 Mafumu 2:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Choncho Bati-seba anapita kwa Mfumu Solomo kuti akauze mfumuyo zofuna za Adoniya.+ Nthawi yomweyo mfumu inaimirira+ kuti ikumane naye ndipo inamuweramira.+ Kenako inakhala pampando wake wachifumu n’kuitanitsa mpando wina ndipo inauika kumbali yake yakumanja kuti amayi a mfumu akhalepo.+ 2 Timoteyo 1:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Pakuti ndikukumbukira chikhulupiriro+ chopanda chinyengo+ chimene uli nacho, chimene chinayamba kukhazikika mwa agogo ako aakazi a Loisi, ndi mayi ako a Yunike, ndipo ndikukhulupirira kuti chilinso mwa iwe.
11 Pamenepo anthu onse ndi akulu amene anali pachipata anayankha kuti: “Ndife mboni! Yehova adalitse mkazi amene akulowa m’nyumba mwako kuti akhale ngati Rakele+ ndi Leya,+ akazi amene anabereka ana a nyumba ya Isiraeli.+ Uonetse kulemekezeka kwako mu Efurata+ ndi kudzipangira dzina m’Betelehemu.+
19 Choncho Bati-seba anapita kwa Mfumu Solomo kuti akauze mfumuyo zofuna za Adoniya.+ Nthawi yomweyo mfumu inaimirira+ kuti ikumane naye ndipo inamuweramira.+ Kenako inakhala pampando wake wachifumu n’kuitanitsa mpando wina ndipo inauika kumbali yake yakumanja kuti amayi a mfumu akhalepo.+
5 Pakuti ndikukumbukira chikhulupiriro+ chopanda chinyengo+ chimene uli nacho, chimene chinayamba kukhazikika mwa agogo ako aakazi a Loisi, ndi mayi ako a Yunike, ndipo ndikukhulupirira kuti chilinso mwa iwe.