Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 25:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Zitatero, anthu onse, kuyambira wamng’ono mpaka wamkulu ndi akuluakulu a magulu ankhondo, ananyamuka n’kupita ku Iguputo,+ chifukwa anayamba kuopa Akasidi.+

  • Yesaya 30:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 amene akupita ku Iguputo+ osafunsira kwa ine,+ ndiponso amene akupita ku Iguputo kuti akapeze chitetezo kwa Farao ndi kukabisala mumthunzi wa Iguputo.+

  • Yeremiya 42:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 ndipo mukapitiriza kunena kuti: “Ife tikupita kukakhala ku Iguputo,+ kumene sitidzaona nkhondo kapena kumva kulira kwa lipenga komanso kumene sitidzasowa chakudya, moti tikupita kukakhala kudziko limenelo,”+

  • Yeremiya 43:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Pamapeto pake anafika ku Iguputo+ chifukwa sanamvere mawu a Yehova ndipo patapita nthawi anakafika ku Tahapanesi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena