Salimo 78:55 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 55 Chifukwa cha iwo anachotsa mitundu ina pang’onopang’ono m’dzikoli,+Ndipo anayesa dzikoli ndi kuligawa kwa iwo kukhala cholowa chawo,+Moti anachititsa mafuko a Isiraeli kukhala m’nyumba zawozawo.+ Ezekieli 47:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Ndiyeno munthu uja anapita mbali ya kum’mawa atatenga chingwe choyezera m’manja mwake.+ Kenako anayeza mtsinjewo mikono 1,000 kuchokera pa Nyumba ija, ndipo anandiuza kuti ndiwoloke mtsinjewo. Madziwo anali olekeza m’mapazi. Zekariya 2:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Tsopano ndinakweza maso ndipo ndinaona munthu ali ndi chingwe choyezera m’dzanja lake.+ Chivumbulutso 11:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Ndiyeno ndinapatsidwa bango lokhala ngati ndodo+ ndipo ndinauzidwa kuti: “Nyamuka, kayeze nyumba yopatulika ya pakachisi+ wa Mulungu, guwa lansembe, ndi amene akulambira mmenemo. Chivumbulutso 21:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Tsopano amene anali kundilankhula uja ananyamula bango+ lagolide loyezera, kuti ayeze mzindawo, zipata zake, ndi mpanda wake.+
55 Chifukwa cha iwo anachotsa mitundu ina pang’onopang’ono m’dzikoli,+Ndipo anayesa dzikoli ndi kuligawa kwa iwo kukhala cholowa chawo,+Moti anachititsa mafuko a Isiraeli kukhala m’nyumba zawozawo.+
3 Ndiyeno munthu uja anapita mbali ya kum’mawa atatenga chingwe choyezera m’manja mwake.+ Kenako anayeza mtsinjewo mikono 1,000 kuchokera pa Nyumba ija, ndipo anandiuza kuti ndiwoloke mtsinjewo. Madziwo anali olekeza m’mapazi.
11 Ndiyeno ndinapatsidwa bango lokhala ngati ndodo+ ndipo ndinauzidwa kuti: “Nyamuka, kayeze nyumba yopatulika ya pakachisi+ wa Mulungu, guwa lansembe, ndi amene akulambira mmenemo.
15 Tsopano amene anali kundilankhula uja ananyamula bango+ lagolide loyezera, kuti ayeze mzindawo, zipata zake, ndi mpanda wake.+