Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 18:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Azitumikira inuyo ndi kugwira ntchito zawo za pachihema chonse.+ Koma asamayandikire zipangizo za m’malo oyera, kapena kuyandikira guwa lansembe kuti iwowo kapena inuyo mungafe.+

  • 2 Mafumu 23:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Koma ansembe+ a malo okwezekawo sankabwera kuguwa lansembe la Yehova ku Yerusalemu. M’malomwake, ankadya mikate yopanda chofufumitsa+ pakati pa abale awo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena