-
Oweruza 16:30Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
30 Ndipo Samisoni anati: “Ndife nawo limodzi+ Afilisitiwa.” Pamenepo anawerama atasonkhanitsa mphamvu zake zonse moti nyumbayo inagwera olamulira ogwirizana a Afilisiti ndi anthu onse amene anali m’nyumbayo.+ Anthu amene Samisoni anawapha pa imfa yake anali ambiri kuposa anthu amene anawapha pa moyo wake.+
-