Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 2:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Koma usadye zipatso za mtengo wodziwitsa chabwino ndi choipa. Chifukwa tsiku limene udzadya, udzafa ndithu.”+

  • Genesis 17:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Mwamuna aliyense wosadulidwa amene sadzadulidwa, ameneyo aphedwe kuti asakhalenso pakati pa anthu ake.+ Waphwanya pangano langa.”

  • Oweruza 16:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Ndipo Samisoni anati: “Ndife nawo limodzi+ Afilisitiwa.” Pamenepo anawerama atasonkhanitsa mphamvu zake zonse moti nyumbayo inagwera olamulira ogwirizana a Afilisiti ndi anthu onse amene anali m’nyumbayo.+ Anthu amene Samisoni anawapha pa imfa yake anali ambiri kuposa anthu amene anawapha pa moyo wake.+

  • Yobu 33:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Iye amayandikira kudzenje,+

      Ndipo moyo wake umayandikira kwa akupha.

  • Salimo 78:50
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 50 Mkwiyo wake anaulambulira njira.+

      Sanawabweze kuwachotsa ku imfa.

      Ndipo anawapha ndi mliri.+

  • Yesaya 53:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pa chifukwa chimenechi, ndidzamupatsa gawo pamodzi ndi ambiri+ ndipo iye adzagawana zolanda ndi amphamvu,+ chifukwa anakhuthula moyo wake mu imfa+ ndipo anaonedwa monga mmodzi wa ochimwa.+ Iye ananyamula tchimo la anthu ambiri+ ndipo analowererapo kuti athandize olakwa.+

  • Machitidwe 3:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Ndithudi, munthu aliyense amene sadzamvera Mneneri ameneyo Mulungu adzamuwononga ndi kumuchotsa pakati pa anthu ake.’+

  • Aroma 6:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Chifukwa malipiro a uchimo ndi imfa,+ koma mphatso+ imene Mulungu amapereka ndi moyo wosatha+ kudzera mwa Khristu Yesu Ambuye wathu.+

  • Chivumbulutso 16:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Mngelo wachiwiri+ anathira mbale yake m’nyanja.+ Ndipo nyanja inasanduka magazi+ ngati a munthu wakufa, moti chamoyo chilichonse m’nyanjamo chinafa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena