Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 61:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Iwo adzamanganso malo amene akhala owonongeka kwa nthawi yaitali.+ Adzamanga malo amene anasakazidwa kalekale.+ Adzakonzanso mizinda yowonongedwa,+ malo amene akhala osakazidwa ku mibadwomibadwo.

  • Yesaya 65:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Iwo adzamanga nyumba n’kukhalamo.+ Adzabzala minda ya mpesa n’kudya zipatso zake.+

  • Ezekieli 36:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 “Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti, ‘Pa tsiku limene ndidzakuyeretseni kuchotsa zolakwa zanu zonse, ndidzachititsanso kuti m’mizinda yanu mukhale anthu+ ndipo malo owonongeka adzamangidwanso.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena