15 Koma ngati nkhani yake ili yokhudza mikangano pa mawu, mayina+ ndi chilamulo+ chanu, zimenezo muthane nazo nokha. Ine sindikufuna kuti ndikhale woweruza nkhani zoterezi.”
19 Iwo anali kungotsutsana naye nkhani zokhudzana ndi kulambira+ kwawo mulungu, ndi za munthu wina wake wotchedwa Yesu amene anafa koma Paulo akupitiriza kunena motsimikiza kuti ali moyo.+