Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Machitidwe 23:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Komabe popeza andiululira za chiwembu+ chimene amukonzera munthuyu, ine ndamutumiza kwa inu msanga, ndipo ndalamula omuimba mlanduwo kuti adzamuneneze mlanduwo pamaso panu.”+

  • Machitidwe 25:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Koma ine ndinawayankha kuti, Aroma sachita zinthu mwa njira imeneyo. Iwo sapereka munthu m’manja mwa omuneneza pongofuna kuwakondweretsa, munthu wonenezedwayo+ asanapatsidwe mwayi woonana pamasom’pamaso ndi omunenezawo kuti alankhule mawu odziteteza pa mlanduwo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena