Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 19
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Deuteronomo 19:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 34:24; Yos 24:8
  • +De 6:10; 7:1; 9:1; 12:29

Deuteronomo 19:2

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 21:13; Nu 35:14; Yos 20:7

Deuteronomo 19:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yos 20:9

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    11/2017, tsa. 14

Deuteronomo 19:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 35:15; De 4:42

Deuteronomo 19:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Mf 6:5
  • +Nu 35:25

Deuteronomo 19:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 35:12, 19; Yos 20:5; 2Sa 14:7
  • +De 17:8; Yos 20:4; 2Mb 19:10

Deuteronomo 19:7

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 19:2

Deuteronomo 19:8

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 15:18; Eks 23:31; De 11:24
  • +Ge 28:14; De 12:20

Deuteronomo 19:9

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 11:22; 12:32; 1Yo 5:3
  • +Yos 20:8

Deuteronomo 19:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 21:9; 2Mf 21:16; Miy 6:17; Yer 7:6; Yon 1:14; Mt 27:4
  • +Sl 5:6; 55:23; Mac 20:26

Deuteronomo 19:11

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mt 15:19; 1Yo 3:15
  • +Eks 21:12; Nu 35:16; De 27:24

Deuteronomo 19:12

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 9:6; 1Mf 2:5, 31

Deuteronomo 19:13

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 19:21
  • +Le 24:17, 21; Nu 35:33; De 21:9; 2Sa 21:1

Deuteronomo 19:14

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 27:17; Yob 24:2; Miy 23:10

Deuteronomo 19:15

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 35:30; De 17:6
  • +1Mf 21:10; Mt 18:16; 26:60; Yoh 8:17; 2Ak 13:1; 1Ti 5:19; Ahe 10:28

Deuteronomo 19:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 23:1; 1Mf 21:13; Sl 27:12; Mko 14:56

Deuteronomo 19:17

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 17:9; 21:5

Deuteronomo 19:18

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 13:14; 17:4; 2Mb 19:6; Yob 29:16

Deuteronomo 19:19

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Miy 19:5; Da 6:24
  • +De 21:21; 24:7; 1Ak 5:13

Deuteronomo 19:20

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 13:11; 17:13; 1Ti 5:20

Deuteronomo 19:21

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 19:13
  • +Eks 21:23; Le 24:20; Mt 5:38

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo,

    Yandikirani, ptsa. 131-133

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Deut. 19:1Eks 34:24; Yos 24:8
Deut. 19:1De 6:10; 7:1; 9:1; 12:29
Deut. 19:2Eks 21:13; Nu 35:14; Yos 20:7
Deut. 19:3Yos 20:9
Deut. 19:4Nu 35:15; De 4:42
Deut. 19:52Mf 6:5
Deut. 19:5Nu 35:25
Deut. 19:6Nu 35:12, 19; Yos 20:5; 2Sa 14:7
Deut. 19:6De 17:8; Yos 20:4; 2Mb 19:10
Deut. 19:7De 19:2
Deut. 19:8Ge 15:18; Eks 23:31; De 11:24
Deut. 19:8Ge 28:14; De 12:20
Deut. 19:9De 11:22; 12:32; 1Yo 5:3
Deut. 19:9Yos 20:8
Deut. 19:10De 21:9; 2Mf 21:16; Miy 6:17; Yer 7:6; Yon 1:14; Mt 27:4
Deut. 19:10Sl 5:6; 55:23; Mac 20:26
Deut. 19:11Mt 15:19; 1Yo 3:15
Deut. 19:11Eks 21:12; Nu 35:16; De 27:24
Deut. 19:12Ge 9:6; 1Mf 2:5, 31
Deut. 19:13De 19:21
Deut. 19:13Le 24:17, 21; Nu 35:33; De 21:9; 2Sa 21:1
Deut. 19:14De 27:17; Yob 24:2; Miy 23:10
Deut. 19:15Nu 35:30; De 17:6
Deut. 19:151Mf 21:10; Mt 18:16; 26:60; Yoh 8:17; 2Ak 13:1; 1Ti 5:19; Ahe 10:28
Deut. 19:16Eks 23:1; 1Mf 21:13; Sl 27:12; Mko 14:56
Deut. 19:17De 17:9; 21:5
Deut. 19:18De 13:14; 17:4; 2Mb 19:6; Yob 29:16
Deut. 19:19Miy 19:5; Da 6:24
Deut. 19:19De 21:21; 24:7; 1Ak 5:13
Deut. 19:20De 13:11; 17:13; 1Ti 5:20
Deut. 19:21De 19:13
Deut. 19:21Eks 21:23; Le 24:20; Mt 5:38
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
  • 18
  • 19
  • 20
  • 21
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Deuteronomo 19:1-21

Deuteronomo

19 “Yehova Mulungu wako akadzawononga mitundu+ ya m’dziko limene Yehova Mulungu wako akukupatsa, iwe n’kuwalandadi dzikolo ndi kukhala m’mizinda yawo ndi m’nyumba zawo,+ 2 udzadzipatulire mizinda itatu pakati pa dziko limene Yehova Mulungu wako akukupatsa kuti likhale lako.+ 3 Udzadzilambulire njira yopita kumizindayo ndipo udzagawe dziko limene Yehova Mulungu wako wakupatsa kuti likhale lako. Dzikolo udzaligawe m’zigawo zitatu. Wopha munthu azithawira kumizinda imeneyo.+

4 “Nkhani ya munthu wopha mnzake amene angathawire kumeneko kuti akhale ndi moyo, izikhala yotere: Akapha munthu mosadziwa ndipo sanali kudana naye,+ 5 kapena akapita ndi mnzake kuthengo kukafuna nkhuni, ndipo wakweza dzanja lake kuti adule mtengo ndi nkhwangwa koma nkhwangwayo yaguluka mumpini wake+ n’kukantha mnzake ndi kumupha, wopha mnzakeyo azithawira ku umodzi mwa mizinda imeneyi kuti akhale ndi moyo.+ 6 Akapanda kutero, wobwezera magazi+ angathamangitse wopha munthuyo ndi kum’peza, chifukwa mtunda ndi wautali. Pamenepo angamukanthe ndi kumupha chifukwa chakuti mtima wake ndi wodzaza ndi ukali, ngakhale kuti wopha mnzake mwangoziyo sanayenere kufa+ chifukwa sanali kudana naye. 7 N’chifukwa chake ndikukulamula kuti, ‘Udzipatulire mizinda itatu.’+

8 “Yehova Mulungu wanu akadzafutukula dera lanu malinga ndi zimene analumbirira makolo anu,+ n’kukupatsani dziko lonse limene analonjeza makolo anu kuti adzawapatsa,+ 9 chifukwa chakuti mwasunga malamulo onsewa amene ndikukupatsani lero mwa kuwatsatira, kuti muzikonda Yehova Mulungu wanu ndi kuyenda m’njira zake nthawi zonse,+ pamenepo mudzawonjezere mizinda inanso itatu pa mizinda imeneyi,+ 10 kuti musakhetse magazi a munthu wosalakwa+ pakati pa dziko lanu limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani monga cholowa, kotero kuti musakhale ndi mlandu wa magazi.+

11 “Koma pakakhala munthu wodana+ ndi mnzake amene wabisalira ndi kuukira mnzakeyo panjira n’kumukantha ndipo wafa,+ iye n’kuthawira ku umodzi mwa mizinda imeneyi, 12 akulu a mumzinda wakwawo azitumiza anthu kukam’tenga kumeneko, ndipo azim’pereka m’manja mwa wobwezera magazi kuti afe ndithu.+ 13 Diso lako lisamumvere chisoni+ ndipo uzichotsa mlandu wa magazi a munthu wosalakwa mu Isiraeli+ kuti zinthu zikuyendere bwino.

14 “Usasunthe zizindikiro za malire a mnzako,+ makolo anu ataika kale malire a cholowa chimene udzalandira, m’dziko limene Yehova Mulungu wako akukupatsa kuti ulitenge kukhala lako.

15 “Munthu akachita tchimo, mboni imodzi si yokwanira kutsimikizira kuti wachitadi cholakwacho kapena tchimo lililonse.+ Muzitsimikizira nkhaniyo mutamva umboni wapakamwa pa mboni ziwiri kapena zitatu.+ 16 Munthu akakonzera mnzake chiwembu mwa kupereka umboni wonama wakuti waphwanya lamulo,+ 17 anthu awiri otsutsanawo aziima pamaso pa Yehova, pamaso pa ansembe ndi oweruza amene aziweruza masiku amenewo.+ 18 Pamenepo oweruza azifufuza nkhaniyo mosamala.+ Mboniyo ikapezeka kuti ndi yonama ndipo yaneneza m’bale wake mlandu wonama, 19 muziichitira zimene inafuna kuti zichitikire m’bale wakezo,+ ndipo muzichotsa woipayo pakati panu.+ 20 Chotero ena onse adzamva ndi kuchita mantha, ndipo sadzachitanso choipa chilichonse ngati chimenechi pakati panu.+ 21 Diso lako lisamumvere chisoni.+ Pazikhala moyo kulipira moyo, diso kulipira diso, dzino kulipira dzino, dzanja kulipira dzanja, phazi kulipira phazi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena