Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 42:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Inu Mulungu wanga, ine ndataya mtima.+

      Nʼchifukwa chake ndakukumbukirani,+

      Pamene ndili mʼdziko la Yorodano ndi mʼmapiri a Herimoni,

      Pamene ndili mʼPhiri la Mizara.*

  • Salimo 62:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Muzimudalira nthawi zonse, anthu inu.

      Mukhuthulireni zonse zamumtima mwanu.+

      Mulungu ndi malo athu othawirako.+ (Selah)

  • Salimo 142:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Ndimakhuthula nkhawa zanga pamaso pake.

      Ndimafotokoza mavuto anga pamaso pake+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena