-
Salimo 18:6Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
6 Pa nthawi ya mavuto anga ndinaitana Yehova,
Ndinapitiriza kufuulira Mulungu wanga kuti andithandize.
-
-
Mateyu 26:38, 39Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
38 Kenako anawauza kuti: “Ine ndikumva chisoni* chofa nacho. Khalani pompano ndipo mukhalebe maso pamodzi ndi ine.”+ 39 Choncho atapita patsogolo pangʼono, anagwada mpaka nkhope yake pansi ndipo anapemphera kuti:+ “Atate wanga, ngati nʼkotheka lolani kuti kapu iyi+ indipitirire. Koma osati mwa kufuna kwanga, koma mwa kufuna kwanu.”+
-