Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 16:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Kenako Kora+ mwana wa Izara,+ mwana wa Kohati,+ mwana wa Levi,+ anagwirizana ndi adzukulu a Rubeni,+ omwe ndi Datani ndi Abiramu ana a Eliyabu,+ komanso Oni mwana wa Pelete, kuti aukire.

  • Numeri 16:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Nthakayo inangʼambika* nʼkuwameza limodzi ndi mabanja awo komanso anthu ena onse amene anali kumbali ya Kora+ pamodzi ndi katundu wawo yense.

  • Numeri 26:10, 11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Zitatero, nthaka inangʼambika* nʼkuwameza. Koma Kora anafa pamene moto unapsereza amuna 250.+ Ndipo iwo anakhala chitsanzo chotichenjeza.+ 11 Koma ana a Kora sanafe.+

  • Yuda 11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ali ndi tsoka chifukwa atsatira njira ya Kaini,+ asankha njira yolakwika ya Balamu+ kuti alandire mphoto ndipo awonongeka polankhula moukira+ ngati Kora.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena