Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 37:39, 40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 Chipulumutso cha anthu olungama chimachokera kwa Yehova.+

      Iye ndi malo awo achitetezo champhamvu pa nthawi ya mavuto.+

      40 Yehova adzawathandiza nʼkuwapulumutsa.+

      Adzawalanditsa kwa oipa nʼkuwapulumutsa,

      Chifukwa athawira kwa iye.+

  • Salimo 50:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Pa nthawi yamavuto mundiitane.+

      Ine ndidzakupulumutsani, ndipo inu mudzandilemekeza.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena