Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 132:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Ansembe ake ndidzawaveka chipulumutso,+

      Ndipo okhulupirika ake adzafuula mosangalala.+

  • Yesaya 61:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ndidzasangalala kwambiri mwa Yehova.

      Ndidzasangalala mwa Mulungu wanga ndi mtima wanga wonse.+

      Chifukwa iye wandiveka zovala zachipulumutso.+

      Wandiveka mkanjo wa chilungamo,*

      Ngati mkwati amene wavala nduwira yofanana ndi ya wansembe,+

      Ndiponso ngati mkwatibwi amene wavala zinthu zake zodzikongoletsera.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena