Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 24:12, 13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Yehova aweruze pakati pa ine ndi inu,+ ndipo Yehova abwezere mʼmalo mwa ine,+ koma dzanja langali silidzakuchitirani choipa.+ 13 Paja mwambi wakale umati, ‘Choipa chimachokera kwa munthu woipa,’ koma dzanja langa silidzakuchitirani choipa.

  • 1 Samueli 26:8-10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndiyeno Abisai anauza Davide kuti: “Lero Mulungu wapereka mdani wanu mʼmanja mwanu.+ Bwanji ndimubaye ndi mkondo nʼkumukhomerera pansi? Ndimubaya kamodzi kokha, sindichita kubwereza kawiri.” 9 Koma Davide anauza Abisai kuti: “Ayi, usamubaye. Ndani angavulaze wodzozedwa wa Yehova+ nʼkukhala wopanda mlandu?”+ 10 Davide anapitiriza kuti: “Ndikulumbira mʼdzina la Yehova, Mulungu wamoyo, Yehova adzamulanga yekha,+ kapena tsiku lidzafika+ ndipo adzamwalira, kapenanso adzapita kunkhondo nʼkukaphedwa.+

  • Salimo 37:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Khala chete pamaso pa Yehova+

      Ndipo umuyembekezere moleza mtima.

      Usakhumudwe ndi munthu

      Amene amakonza ziwembu nʼkuzikwaniritsa popanda vuto lililonse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena