Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 90:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Mapiri asanabadwe,

      Kapena musanakhazikitse dziko lapansi komanso nthaka,+

      Inu ndinu Mulungu kuyambira kalekale mpaka kalekale.+

  • Danieli 7:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ndinapitiriza kuyangʼana mpaka pamene mipando yachifumu inaikidwa ndipo Wamasiku Ambiri+ anakhala pampando wake wachifumu.+ Zovala zake zinali zoyera kwambiri+ ndipo tsitsi lake linali looneka ngati ubweya wa nkhosa woyera. Mpando wake wachifumu unkaoneka ngati malawi a moto ndipo mawilo a mpandowo ankaoneka ngati moto umene ukuyaka.+

  • Danieli 7:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndinapitiriza kuona masomphenya usikuwo ndipo ndinaona winawake wooneka ngati mwana wa munthu+ akubwera mʼmitambo. Iye analoledwa kufika kwa Wamasiku Ambiri+ uja ndipo anamubweretsa pafupi kwambiri ndi Wamasiku Ambiriyo.

  • Habakuku 1:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Inu Yehova, mwakhala mulipo kuyambira kalekale.+

      Inu Mulungu wanga, Mulungu wanga Woyera, inu simufa.*+

      Inu Yehova, mwasankha Akasidi kuti apereke chiweruzo chanu.

      Inu Thanthwe langa,+ mwawasankha kuti mupereke chilango.*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena