Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 40:3-5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Winawake akufuula mʼchipululu kuti:

      “Konzani njira ya Yehova!+

      Mulungu wathu mukonzereni msewu wowongoka+ wodutsa mʼchipululu.+

       4 Chigwa chilichonse chikwezedwe mʼmwamba,

      Ndipo phiri lililonse ndi chitunda chilichonse zitsitsidwe.

      Malo okumbikakumbika asalazidwe,

      Ndipo malo azitunda akhale chigwa.+

       5 Ulemerero wa Yehova udzaonekera,+

      Ndipo anthu onse adzauonera limodzi,+

      Chifukwa pakamwa pa Yehova panena.”

  • Luka 2:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 chifukwa maso anga aona njira yanu yopulumutsira anthu+

  • Machitidwe 28:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Choncho dziwani kuti njira ya Mulungu yopulumutsira anthu, yatumizidwa kwa anthu a mitundu ina.+ Ndipo mosakayikira, iwo adzamvetsera.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena