Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 10:19, 20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Koma akadzakupititsani kumeneko, musadzade nkhawa kuti mudzalankhula bwanji kapena kuti mudzanena chiyani, chifukwa zoti mulankhule mudzapatsidwa nthawi yomweyo.+ 20 Zili choncho chifukwa wolankhula simudzakhala inu nokha, koma mzimu wa Atate wanu udzalankhula kudzera mwa inu.+

  • Maliko 13:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Koma pamene akupita nanu kukakuperekani, musafulumire kuda nkhawa kuti mukanena chiyani. Zimene mukapatsidwe mu ola lomwelo, mukanene zomwezo chifukwa wolankhula si inu, koma mzimu woyera.+

  • Luka 21:14, 15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Choncho tsimikizirani mʼmitima yanu kuti musachite kukonzekera zoti mukayankhe podziteteza,+ 15 chifukwa ine ndidzakuuzani mawu oti munene komanso ndidzakupatsani nzeru zimene otsutsa anu onse sadzatha kuzikana kapena kuzitsutsa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena