Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 9/09 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa September 28

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa September 28
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA SEPTEMBER 28
Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
km 9/09 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa September 28

MLUNGU WOYAMBIRA SEPTEMBER 28

Nyimbo Na. 186

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl-CN mutu 26 ndime 16-23 ndi bokosi la patsamba 269

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Numeri 33-36

Na. 1: Numeri 33:1-23

Na. 2: Tingauke kwa Akufa! (lr-CN mutu 35)

Na. 3: Kodi Ufumu wa Mulungu Umaposa Maboma a Anthu M’njira Ziti?

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 21

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Kugwiritsa Ntchito Mafanizo Pophunzitsa. Nkhani yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, masamba 240-243.

Mph. 20: “Fufuzani Anthu Oyenerera.” Kambiranani mwa mafunso ndi mayankho. Funsani wofalitsa mmodzi kapena awiri amene amayesetsa kulalikira pogwiritsa ntchito njira zosiyanasiyana.

Nyimbo Na. 126

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena