Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 May tsamba 6
  • Zimene Maulosi Ananena Zokhudza Mesiya

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Maulosi Ananena Zokhudza Mesiya
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Maulosi Onena za Mesiya Amatsimikizira Kuti Yesu Analidi Mesiya?
    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
  • Yesu Ndi Mesiya Amene Mulungu Ananeneratu Kuti Adzabwera
    Kodi Baibulo Limaphunzitsa Chiyani Kwenikweni?
  • Mafunso Ochokera kwa Owerenga
    Nsanja ya Olonda—1987
  • Kupanga Dziko Limodzi Pansi pa Ufumu wa Mulungu
    Mbiri Yabwino Yokusangalatsani
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 May tsamba 6

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MASALIMO 19-25

Zimene Maulosi Ananena Zokhudza Mesiya

LEMBA

ULOSI

KUKWANIRITSIDWA KWAKE

Salimo 22:1

Anaoneka ngati wasiyidwa ndi Mulungu

Mateyu 27:46; Maliko 15:34

Salimo 22:7, 8

Ananyozedwa ali pamtengo wozunzikirapo

Mateyu 27:39-43

Salimo 22:16

Anamukhomerera pamtengo

Mateyu 27:31; Maliko 15:25; Yohane 20:25

Salimo 22:18

Anachita mayere pazovala zake

Mateyu 27:35

Salimo 22:22

Anatsogolera pa ntchito yolalikira za dzina la Yehova

Yohane 17:6

Munthu wonyoza akumenya mbama Yesu; kenako anthu akulira pamene Yesu akutsirizika pamtengo wozunzikirapo
    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena