Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 12/11 tsamba 3
  • Zimene Tingachite Kuti Tizisangalala ndi Nyimbo za Ufumu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Tingachite Kuti Tizisangalala ndi Nyimbo za Ufumu
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • Nkhani Yofanana
  • Nyimbo Zimene Zimatsitsimula
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2004
  • Imbirani Yehova
    Nsanja ya Olonda—2010
  • Kodi Ndimotani Mmene Ndingasungire Nyimbo m’Malo Ake?
    Galamukani!—1993
  • Kodi Ndingatani Kuti Ndisamangokhalira Kumvetsera Nyimbo?
    Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa, Buku Lachiwiri
Onani Zambiri
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 12/11 tsamba 3

Zimene Tingachite Kuti Tizisangalala ndi Nyimbo za Ufumu

Atumiki a Mulungu amaona kuti nyimbo ndi mphatso yabwino kwambiri yochokera kwa Mulungu. (Yak. 1:17) M’mipingo yambiri, abale amasangalala kumvetsera Nyimbo za Ufumu zimene zimaimbidwa chapansipansi misonkhano isanayambe kapena ikatha. Kumvetsera nyimbo zauzimu kumatitsitsimula tikamafika pa misonkhano. Zimatithandiza kukonzekeretsa maganizo pa nkhani yolambira. Komanso kumvetsera nyimbo zatsopano za m’buku la nyimbo kumatithandiza kuzolowera kaimbidwe kake ndipo zimenezi zimatithandizanso kuti tiziimba bwino. Nyimbo za Ufumu zimene zimaimbidwa misonkhano ikatha zimakhala zotsitsimulanso pamene tikucheza ndiponso kulimbikitsana ndi abale athu. Choncho, bungwe lililonse la akulu likonze zoti pampingopo azimvetsera nyimbo za zipangizo zokha za Sing to Jehovah—Piano Accompaniment misonkhano isanayambe kapena ikatha. Koma ayenera kuonetsetsa kuti nyimbozi sizikukwera mawu kwambiri moti n’kulepheretsa abale kucheza bwinobwino.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena