Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 22
  • Ufumu Umene Ukulamulira Kumwamba Ubwere

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ufumu Umene Ukulamulira Kumwamba Ubwere
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Ufumu Umene Ukulamulira Kumwamba Ubwere
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Yehova Ndi Mfumu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Yehova ndi Mfumu Yathu
    Imbirani Yehova
  • ‘Yehova Iye Mwini Wakhala Mfumu!’
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 22

NYIMBO 22

Ufumu Umene Ukulamulira Kumwamba Ubwere

Losindikizidwa

(Chivumbulutso 11:15; 12:10)

  1. 1. Yehova Mulungu wathu

    Ndinu wamuyaya.

    Mwapatsa Yesu Ufumu

    Mwa kufuna kwanu.

    Yesu adzalamulira

    Padziko lonse lapansi.

    (KOLASI)

    Tsopano yafika

    Nthawi ya chipulumutso.

    Ufumu wayamba

    Tikupemphatu: “Ubwere!”

  2. 2. Nthawi ya Satana itha

    Posachedwa pompa.

    Mavuto onse adzatha

    M’dziko latsopano.

    Yesu adzalamulira

    Padziko lonse lapansi.

    (KOLASI)

    Tsopano yafika

    Nthawi ya chipulumutso.

    Ufumu wayamba

    Tikupemphatu: “Ubwere!”

  3. 3. Angelo onse kumwamba

    Akusangalala.

    Satana wachotsedwako

    Kulitu mtendere.

    Yesu adzalamulira

    Padziko lonse lapansi.

    (KOLASI)

    Tsopano yafika

    Nthawi ya chipulumutso.

    Ufumu wayamba

    Tikupemphatu: “Ubwere!”

(Onaninso Dan. 2:​34, 35; 2 Akor. 4:​18.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena