LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 9/15 tsa. 4
  • Maulaliki Acitsanzo

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Maulaliki Acitsanzo
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Nkhani Zofanana
  • Maulaliki Acitsanzo
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Maulaliki Acitsanzo
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Maulaliki Acitsanzo
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Maulaliki Acitsanzo
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
Onaninso Zina
Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
km 9/15 tsa. 4

Maulaliki Acitsanzo

Nsanja ya Mlonda September-October

“Mukaona mavuto amene timakumana nao paumoyo, kodi muganiza kuti mau a Yesu akuti tisade nkhawa ndi othandiza? [Ŵelengani Mateyu 6:25, ndipo yembekezani ayankhe.] Magazini ya Nsanja ya Mlonda iyi ifotokoza mmene kugwilitsila nchito mfundo za m’Baibulo kungakuthandizileni kucepetsa nkhawa zokhudza ndalama, mavuto a m’banja ndi mavuto aumwini.”

Galamukani! October

“Tikuceza ndi anthu mwacidule kaamba kakuti ambili amadzifunsa cifukwa cake Mulungu amalola anthu kuvutika. Kodi mukuona kuti kufunsa Mulungu funso limeneli n’kupanda ulemu? [Yembekezani ayankhe.] Munthu wokhulupilika Yobu nayenso anafuna kufunsa Mulungu. [Ŵelengani Yobu 23:3-5.] Magaziniyi ikufotokoza mafunso atatu amene anthu ambili angakonde kufunsa Mulungu, ngati angakhale ndi mpata wocita zimenezo. Ndipo ikufotokozanso mayankho okhutilitsa a m’Baibulo.”

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani