LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 November tsa. 2
  • “Kodi Umandikonda Ine Kuposa Izi?”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Kodi Umandikonda Ine Kuposa Izi?”
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Nkhani Zofanana
  • Pangani Mbili Yabwino Ndipo Isungeni
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Yehova Amakwanilitsa Malonjezo Ake Nthawi Zonse
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Kusakhulupilika—Khalidwe Loipa Kwambili!
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Kodi Ndimwe Wokonzeka Kukhala Msodzi wa Anthu?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2020
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 November tsa. 2
Ophunzila a Yesu akudonsela ku mtunda ukonde wodzala na nsomba

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YOHANE 20-21

“Kodi Umandikonda Ine Kuposa Izi?”

21:1-19

Nthawi za m’Baibo, asodzi oleza mtima, akhama, komanso okonzeka kupilila mavuto pa nchito yawo anali kugwila nsomba zambili. (w12 8/1 mape. 18-20) Makhalidwe amenewa anali othandiza kwa Petulo kuti akhale msodzi wabwino wa anthu. Komabe, iye anafunika kusankha cimene adzaika patsogolo mu umoyo wake, kaya nchito yake yakuthupi imene anali kukonda kapena nchito yauzimu yodyetsa otsatila a Yesu.

Ni zinthu ziti zimene mwasintha mu umoyo wanu kuti muike zinthu za Ufumu patsogolo?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani