Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nehemiya 9:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Munawapatsanso mkate wochokera kumwamba kuti athetse njala yawo.+ Munatulutsa madzi pathanthwe ndi kuwapatsa kuti athetse ludzu lawo,+ ndiyeno munawauza kuti alowe+ ndi kutenga dziko limene munalumbira mutakweza dzanja lanu kuti mudzawapatsa.+

  • Salimo 78:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Iye anang’amba miyala m’chipululu+

      Kuti awapatse madzi akumwa ochuluka ngati a m’nyanja.+

  • Salimo 105:41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 Anatsegula thanthwe ndipo panatuluka madzi ambiri.+

      Madziwo anayenda ngati mtsinje kudutsa m’dera lopanda madzi.+

  • Salimo 114:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Amene amasintha thanthwe kukhala dambo la madzi,+

      Ndiponso amasintha mwala wa nsangalabwi kukhala kasupe.+

  • Yesaya 43:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Zilombo zakutchire zidzanditamanda.+ Mimbulu ndi nthiwatiwa+ zidzanditamanda chifukwa ndidzapereka madzi ndi mitsinje m’chipululu,+ kuti anthu anga, wosankhidwa wanga,+ amwe,

  • Yesaya 48:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Iwo sanamve ludzu+ ngakhale pamene iye anawayendetsa m’chipululu.+ Iye anawatulutsira madzi pathanthwe. Anang’amba thanthwe kuti madzi atulukepo.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena