Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 49:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ndodo yachifumu sidzachoka kwa Yuda,+ ndiponso chibonga cha wolamulira sichidzachoka pakati pa mapazi ake, kufikira Silo*+ atabwera. Ndipo mitundu ya anthu idzamumvera.+

  • Salimo 2:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Mitunduyo udzaiswa ndi ndodo yachifumu yachitsulo,+

      Udzaiphwanya ngati mbiya yadothi, n’kukhala zidutswazidutswa.”+

  • Salimo 72:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Mafumu onse adzamugwadira ndi kumuweramira.+

      Ndipo mitundu yonse ya anthu idzamutumikira.+

  • Chivumbulutso 6:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Nditayang’ana, ndinaona hatchi* yoyera.+ Wokwerapo+ wake ananyamula uta.+ Iye anapatsidwa chisoti chachifumu,+ ndi kupita kukagonjetsa adani ake+ ndipo anapambana pa nkhondo yolimbana nawo.+

  • Chivumbulutso 19:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 M’kamwa mwake munali kutuluka lupanga+ lalitali lakuthwa, loti aphere mitundu ya anthu, ndipo adzawakusa ndi ndodo yachitsulo.+ Iye anali kupondapondanso m’chopondera mphesa+ cha mkwiyo waukulu wa Mulungu+ Wamphamvuyonse.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena