Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 13:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Choncho amunawo anapita kukazonda dzikolo, kuyambira kuchipululu cha Zini+ mpaka ku Rehobu,+ kufupi ndi Hamati.+

  • Numeri 14:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Popeza kuti Aamaleki ndi Akanani+ akukhala kuchigwa, mawa mutembenuke, munyamuke ulendo wolowera kuchipululu podzera njira yopita ku Nyanja Yofiira.”+

  • Numeri 20:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Tsopano khamu lonse la ana a Isiraeli linafika m’chipululu cha Zini,+ m’mwezi woyamba, ndipo anthuwo anakhala ku Kadesi.+ Kumeneko n’kumene Miriamu+ anafera n’kuikidwa m’manda.

  • Numeri 27:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 chifukwa amuna inu munapandukira mawu anga m’chipululu cha Zini, pa nthawi imene khamu lija linakangana nanu.+ Munalephera kundilemekeza+ pa madzi amene anatuluka patsogolo pa khamulo, madzi a Meriba+ ku Kadesi,+ m’chipululu cha Zini.”+

  • Deuteronomo 32:51
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 51 Izi zili choncho chifukwa anthu inu munachita mosakhulupirika kwa ine+ pakati pa ana a Isiraeli, kumadzi a pa Meriba+ ku Kadesi, m’chipululu cha Zini. Ndiponso chifukwa chakuti anthu inu simunandilemekeze pakati pa ana a Isiraeli.+

  • Yoswa 15:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Gawo+ la fuko la ana a Yuda potsata mabanja awo linkafika kumalire a Edomu,+ ndi kuchipululu cha Zini,+ mpaka kothera kwa Negebu,+ kum’mwera.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena