2 Samueli 23:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Mzimu wa Yehova unandilankhulitsa,+Ndipo mawu ake anali palilime langa.+ 1 Mafumu 2:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Adoniya anapitiriza kuti: “Inu mukudziwa bwino kuti ufumu unayenera kukhala wanga, ndipo Aisiraeli onse maso awo anali pa ine kuti ndikhala mfumu.+ Koma ufumuwo unatembenuka n’kukhala wa m’bale wanga, chifukwa Yehova ndiye anam’patsa ufumuwo kuti ukhale wake.+ 1 Mafumu 2:24 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 24 Tsopano m’dzina la Yehova Mulungu wamoyo,+ amene wandichititsa kukhazikika,+ amene wandiika pampando wachifumu wa Davide bambo anga,+ ndiponso amene anandipatsa mzere wa banja lachifumu+ monga ananenera,+ lero Adoniya aphedwa.”+ 1 Mbiri 29:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 29 Tsopano mfumu Davide inauza mpingo wonse+ kuti: “Solomo mwana wanga, amene Mulungu wamusankha,+ ndi wamng’ono+ ndi wosakhwima. Koma ntchitoyi ndi yaikulu chifukwa chinyumba chachikuluchi, si cha munthu ayi,+ koma ndi cha Yehova Mulungu.
15 Adoniya anapitiriza kuti: “Inu mukudziwa bwino kuti ufumu unayenera kukhala wanga, ndipo Aisiraeli onse maso awo anali pa ine kuti ndikhala mfumu.+ Koma ufumuwo unatembenuka n’kukhala wa m’bale wanga, chifukwa Yehova ndiye anam’patsa ufumuwo kuti ukhale wake.+
24 Tsopano m’dzina la Yehova Mulungu wamoyo,+ amene wandichititsa kukhazikika,+ amene wandiika pampando wachifumu wa Davide bambo anga,+ ndiponso amene anandipatsa mzere wa banja lachifumu+ monga ananenera,+ lero Adoniya aphedwa.”+
29 Tsopano mfumu Davide inauza mpingo wonse+ kuti: “Solomo mwana wanga, amene Mulungu wamusankha,+ ndi wamng’ono+ ndi wosakhwima. Koma ntchitoyi ndi yaikulu chifukwa chinyumba chachikuluchi, si cha munthu ayi,+ koma ndi cha Yehova Mulungu.