Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 37:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Oipa asolola lupanga ndipo akunga uta wawo,+

      Kuti agwetse osautsika ndi osauka,+

      Kuti aphe anthu amene njira zawo ndi zowongoka.+

  • Miyambo 1:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Chotero anthu ochimwa amabisala kuti akhetse magazi a anthu ena.+ Amabisalira miyoyo ya anthu ena.+

  • Miyambo 21:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Munthu amene amadzikuza akapsa mtima, amatchedwa wodzikuza, wonyada ndi wodzitama.+

  • Miyambo 27:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Mkwiyo umasefukira ndipo ukali ndi wankhanza,+ koma nsanje ndani angaipirire?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena