Esitere 3:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Pamenepo mfumu inavula mphete yodindira+ kudzanja lake ndi kuipereka kwa Hamani+ mwana wa Hamedata Mwagagi,+ amene anali kudana kwambiri ndi Ayuda.+ Esitere 8:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Choncho Mfumu Ahasiwero inauza mfumukazi Esitere ndi Moredekai Myuda kuti: “Nyumba ya Hamani ndaipereka kwa Esitere,+ ndipo Hamani wapachikidwa pamtengo+ chifukwa chakuti anatambasula dzanja lake ndi kuukira Ayuda. Esitere 9:24 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 24 Izi zinali choncho chifukwa Hamani+ mwana wa Hamedata+ Mwagagi,+ amene anali kudana+ ndi Ayuda onse, anakonzera Ayudawo chiwembu kuti awawononge.+ Choncho iye anachita Puri+ kapena kuti Maere,+ ndi cholinga chakuti awasautse ndi kuwawononga.
10 Pamenepo mfumu inavula mphete yodindira+ kudzanja lake ndi kuipereka kwa Hamani+ mwana wa Hamedata Mwagagi,+ amene anali kudana kwambiri ndi Ayuda.+
7 Choncho Mfumu Ahasiwero inauza mfumukazi Esitere ndi Moredekai Myuda kuti: “Nyumba ya Hamani ndaipereka kwa Esitere,+ ndipo Hamani wapachikidwa pamtengo+ chifukwa chakuti anatambasula dzanja lake ndi kuukira Ayuda.
24 Izi zinali choncho chifukwa Hamani+ mwana wa Hamedata+ Mwagagi,+ amene anali kudana+ ndi Ayuda onse, anakonzera Ayudawo chiwembu kuti awawononge.+ Choncho iye anachita Puri+ kapena kuti Maere,+ ndi cholinga chakuti awasautse ndi kuwawononga.