Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 2:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Onse olimbana ndi Yehova adzagwidwa ndi mantha.+

      Motsutsana nawo, iye adzagunda ngati mabingu kumwamba.+

      Yehova mwiniwake adzaweruza dziko lonse lapansi,+

      Kuti apereke mphamvu kwa mfumu yake,+

      Ndi kuti akweze nyanga ya wodzozedwa wake.”+

  • Salimo 75:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Mulungu akuti:* “Ndidzadula nyanga zonse za anthu oipa.”+

      Koma nyanga za munthu wolungama zidzakwezedwa.+

  • Salimo 92:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Koma inu mudzakweza nyanga* yanga ngati nyanga ya ng’ombe yam’tchire yamphongo.*+

      Ndidzadzola mafuta abwino.+

  • Salimo 132:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Ku Ziyoniko ndidzakulitsa nyanga* ya Davide.+

      Wodzozedwa wanga ndamukonzera nyale.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena