Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 15:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Mdaniyo anati, ‘Ndiwathamangira,+ ndi kuwapeza!+

      Ndigawa chuma chawo.+ Pamenepo moyo wanga ukhutira ndi zimene ndawachita!

      Ndisolola lupanga langa! Dzanja langa liwawononga!’+

  • Salimo 146:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Mzimu* wake umachoka,+ ndipo iye amabwerera kunthaka.+

      Pa tsiku limenelo zonse zimene anali kuganiza zimatheratu.+

  • Mlaliki 9:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Pakuti amoyo amadziwa kuti adzafa,+ koma akufa sadziwa chilichonse.+ Iwo salandiranso malipiro alionse, chifukwa zonse zimene anthu akanawakumbukira nazo zaiwalika.+

  • Luka 12:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Koma Mulungu anamuuza kuti, ‘Wopanda nzeru iwe, usiku womwe uno moyo wako adzaufuna.+ Nanga chuma chimene waunjikachi chidzakhala cha ndani?’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena