Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 45:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Ndiwedi wokongola kwambiri kuposa ana a anthu.+

      Mawu otuluka m’kamwa mwako ndi osangalatsadi.+

      N’chifukwa chake Mulungu adzakupatsa madalitso mpaka kalekale.+

  • Nyimbo ya Solomo 5:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 “Wachikondi wanga ndi wokongola ndipo khungu lake ndi lofiirira. Pa amuna 10,000, iye ndiye wooneka bwino kwambiri.+

  • Yohane 1:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Choncho Mawu ameneyo anakhala ndi thupi+ la nyama ndi kukhala pakati pathu, ndipo tinaona ulemerero wake, ulemerero wa mwana wobadwa yekha+ kwa bambo ake. Anali wodzaza ndi kukoma mtima kwakukulu ndi choonadi.+

  • Aheberi 11:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Mwa chikhulupiriro, Mose atabadwa, makolo ake anamubisa kwa miyezi itatu,+ chifukwa anaona kuti mwanayo anali wokongola.+ Iwo sanaope lamulo+ la mfumu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena