Ezekieli 14:23 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 23 “‘Ndithu iwo adzakutonthozani mukadzaona njira zawo ndi zochita zawo. Chotero mudzadziwa kuti zonse zimene ndidzachitire mzindawo, sindinazichite popanda chifukwa,’ watero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa.”+ Ezekieli 33:29 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 29 Dzikolo ndikadzalisandutsa bwinja ndiponso malo owonongeka+ chifukwa cha zonyansa zonse zimene achita,+ iwo adzadziwa kuti ine ndine Yehova.”’ Danieli 9:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Inu munachitadi zimene munachenjeza kuti mudzatichitira,+ ifeyo ndi atsogoleri athu.+ Munatigwetsera tsoka lalikulu ndipo tsoka limene lagwera Yerusalemu silinachitikeponso padziko lonse lapansi.+ Zekariya 1:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Kodi zimene ndinalamula atumiki anga aneneri+ m’mawu anga ndi m’malangizo anga, sizinawachitikire makolo anu?’+ Chotero iwo anabwerera kwa ine ndi kunena kuti: ‘Yehova wa makamu watichitira zimene anakonza kuti atichitire+ mogwirizana ndi njira zathu ndi zochita zathu.’”+
23 “‘Ndithu iwo adzakutonthozani mukadzaona njira zawo ndi zochita zawo. Chotero mudzadziwa kuti zonse zimene ndidzachitire mzindawo, sindinazichite popanda chifukwa,’ watero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa.”+
29 Dzikolo ndikadzalisandutsa bwinja ndiponso malo owonongeka+ chifukwa cha zonyansa zonse zimene achita,+ iwo adzadziwa kuti ine ndine Yehova.”’
12 Inu munachitadi zimene munachenjeza kuti mudzatichitira,+ ifeyo ndi atsogoleri athu.+ Munatigwetsera tsoka lalikulu ndipo tsoka limene lagwera Yerusalemu silinachitikeponso padziko lonse lapansi.+
6 Kodi zimene ndinalamula atumiki anga aneneri+ m’mawu anga ndi m’malangizo anga, sizinawachitikire makolo anu?’+ Chotero iwo anabwerera kwa ine ndi kunena kuti: ‘Yehova wa makamu watichitira zimene anakonza kuti atichitire+ mogwirizana ndi njira zathu ndi zochita zathu.’”+