Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 5:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Chifukwa chakuti Yuda+ anali wamphamvu pakati pa abale ake, mwa iye munachokera mtsogoleri,+ koma udindo wa woyamba kubadwa unali wa Yosefe.+

  • Yesaya 55:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Taonani! Ine ndamupereka+ iye monga mboni+ kwa mitundu ya anthu,+ ndiponso monga mtsogoleri+ ndi wolamulira+ wa mitundu ya anthu.

  • Danieli 9:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Choncho iwe uyenera kudziwa ndi kuzindikira kuti kuchokera pamene mawu adzamveka+ onena kuti Yerusalemu akonzedwe ndi kumangidwanso,+ kufika pamene Mesiya+ Mtsogoleri+ adzaonekere, padzadutsa milungu 7, komanso milungu 62.+ Yerusalemu adzakonzedwa ndi kumangidwanso, ndipo adzakhala ndi bwalo ndi ngalande yachitetezo. Zimenezi zidzachitika mu nthawi zovuta.

  • Yohane 1:49
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 49 Natanayeli anamuyankha kuti: “Rabi, ndinudi Mwana wa Mulungu,+ ndinu Mfumu+ ya Isiraeli.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena