Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Akorinto 6:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 ngati osadziwika koma odziwika bwino,+ ngati oti tikufa koma tikukhalabe ndi moyo,+ ngati olangidwa+ koma osakaphedwa,+

  • 2 Akorinto 11:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Katatu anandimenya ndi ndodo.+ Kamodzi anandiponya miyala.+ Chombo chinandiswekerapo katatu.+ Kamodzi ndinakhala pamadzi akuya usiku ndi usana wonse.

  • 2 Timoteyo 3:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ukudziwanso mazunzo ndi masautso amene ndinakumana nawo ku Antiokeya,+ ku Ikoniyo,+ ndi ku Lusitara.+ Komabe, Ambuye anandipulumutsa m’mazunzo onsewa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena