Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 29
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Deuteronomo 29:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 24:8; Le 26:45; De 5:2

Deuteronomo 29:2

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 19:4; De 7:18; Yos 24:5

Deuteronomo 29:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 4:34; 7:19; Ne 9:17, 19
  • +Nu 14:11
  • +Ne 9:10; Sl 78:43; 105:27

Deuteronomo 29:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Miy 20:12; Yes 6:10; Mko 4:12; Aro 11:8; Aef 4:18

Deuteronomo 29:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 1:3; 8:2; Amo 2:10
  • +De 8:4; Ne 9:21; Mt 6:31

Deuteronomo 29:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 16:12, 31; Ne 9:15

Deuteronomo 29:7

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 21:26
  • +Nu 21:33
  • +Sl 135:10, 11

Deuteronomo 29:8

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 32:33; De 3:12

Deuteronomo 29:9

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 4:6; 8:18; Yos 1:7; 1Mf 2:3; Sl 103:17, 18; Lu 11:28

Deuteronomo 29:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 31:12

Deuteronomo 29:11

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ne 8:2
  • +Eks 12:38; Nu 11:4
  • +Yos 9:21

Deuteronomo 29:12

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 29:1, 29
  • +De 1:3

Deuteronomo 29:13

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 19:5; De 7:6; 27:9; 28:9
  • +Eks 6:7; 29:45
  • +Ge 17:7; 22:16; Yer 11:5; Ahe 6:13
  • +Ge 26:3; Eks 2:24; Sl 105:9
  • +Ge 28:13

Deuteronomo 29:14

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 5:3; Eze 16:60

Deuteronomo 29:15

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yer 32:39

Deuteronomo 29:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 2:4

Deuteronomo 29:17

Mawu a M'munsi

  • *

    Mawu amene ali m’mipukutu yoyambirira pa mawu akuti “onyansa” amatanthauza “ndowe.”

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 25:2; Eze 20:8

Deuteronomo 29:18

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 11:16; 17:3; Ahe 3:12
  • +Yer 9:15; Ho 10:4; Amo 6:12; Mac 8:23; Ahe 12:15

Deuteronomo 29:19

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 29:12
  • +Sl 10:6; Yer 5:12; 14:19
  • +Ne 9:29; Miy 28:14; Yes 30:1; Yer 3:17; 6:28; Zek 7:12; Aro 1:21; 2:5

Deuteronomo 29:20

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 34:7; Yos 24:19; Yes 27:11
  • +Sl 74:1
  • +Eks 34:14; Sl 79:5; Eze 23:25
  • +Sl 18:8; Ahe 12:29
  • +De 27:26; 28:15

Deuteronomo 29:21

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Aro 2:5

Deuteronomo 29:22

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 28:59

Deuteronomo 29:23

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Owe 9:45; Sl 107:34; Yer 17:6
  • +Sl 11:6
  • +Ge 19:24; Yuda 7
  • +Ge 10:19
  • +Ge 14:2; Ho 11:8
  • +Yer 20:16; Amo 4:11

Deuteronomo 29:24

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Mf 9:8; 2Mb 7:21; Yer 22:8

Deuteronomo 29:25

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 29:12; 1Mf 19:10
  • +Yer 22:9; 31:32

Deuteronomo 29:26

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Owe 2:12; 1Mf 9:9; 2Mf 17:7; 2Mb 7:22; Yer 19:4

Deuteronomo 29:27

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 26:16; De 27:26; 29:20

Deuteronomo 29:28

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 28:63; 1Mf 14:15; 2Mf 17:18; Sl 52:5; Lu 21:24
  • +Eza 9:7; Da 9:7

Deuteronomo 29:29

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yes 55:8; Aro 11:33; 1Ak 2:16
  • +Amo 3:7; Mt 11:27; Aef 3:5
  • +Sl 78:5; Mla 12:13; 1Yo 5:3

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    5/15/1987, tsa. 31

    5/15/1986, ptsa. 9-10

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Deut. 29:1Eks 24:8; Le 26:45; De 5:2
Deut. 29:2Eks 19:4; De 7:18; Yos 24:5
Deut. 29:3De 4:34; 7:19; Ne 9:17, 19
Deut. 29:3Nu 14:11
Deut. 29:3Ne 9:10; Sl 78:43; 105:27
Deut. 29:4Miy 20:12; Yes 6:10; Mko 4:12; Aro 11:8; Aef 4:18
Deut. 29:5De 1:3; 8:2; Amo 2:10
Deut. 29:5De 8:4; Ne 9:21; Mt 6:31
Deut. 29:6Eks 16:12, 31; Ne 9:15
Deut. 29:7Nu 21:26
Deut. 29:7Nu 21:33
Deut. 29:7Sl 135:10, 11
Deut. 29:8Nu 32:33; De 3:12
Deut. 29:9De 4:6; 8:18; Yos 1:7; 1Mf 2:3; Sl 103:17, 18; Lu 11:28
Deut. 29:10De 31:12
Deut. 29:11Ne 8:2
Deut. 29:11Eks 12:38; Nu 11:4
Deut. 29:11Yos 9:21
Deut. 29:12De 29:1, 29
Deut. 29:12De 1:3
Deut. 29:13Eks 19:5; De 7:6; 27:9; 28:9
Deut. 29:13Eks 6:7; 29:45
Deut. 29:13Ge 17:7; 22:16; Yer 11:5; Ahe 6:13
Deut. 29:13Ge 26:3; Eks 2:24; Sl 105:9
Deut. 29:13Ge 28:13
Deut. 29:14De 5:3; Eze 16:60
Deut. 29:15Yer 32:39
Deut. 29:16De 2:4
Deut. 29:17Nu 25:2; Eze 20:8
Deut. 29:18De 11:16; 17:3; Ahe 3:12
Deut. 29:18Yer 9:15; Ho 10:4; Amo 6:12; Mac 8:23; Ahe 12:15
Deut. 29:19De 29:12
Deut. 29:19Sl 10:6; Yer 5:12; 14:19
Deut. 29:19Ne 9:29; Miy 28:14; Yes 30:1; Yer 3:17; 6:28; Zek 7:12; Aro 1:21; 2:5
Deut. 29:20Eks 34:7; Yos 24:19; Yes 27:11
Deut. 29:20Sl 74:1
Deut. 29:20Eks 34:14; Sl 79:5; Eze 23:25
Deut. 29:20Sl 18:8; Ahe 12:29
Deut. 29:20De 27:26; 28:15
Deut. 29:21Aro 2:5
Deut. 29:22De 28:59
Deut. 29:23Owe 9:45; Sl 107:34; Yer 17:6
Deut. 29:23Sl 11:6
Deut. 29:23Ge 19:24; Yuda 7
Deut. 29:23Ge 10:19
Deut. 29:23Ge 14:2; Ho 11:8
Deut. 29:23Yer 20:16; Amo 4:11
Deut. 29:241Mf 9:8; 2Mb 7:21; Yer 22:8
Deut. 29:25De 29:12; 1Mf 19:10
Deut. 29:25Yer 22:9; 31:32
Deut. 29:26Owe 2:12; 1Mf 9:9; 2Mf 17:7; 2Mb 7:22; Yer 19:4
Deut. 29:27Le 26:16; De 27:26; 29:20
Deut. 29:28De 28:63; 1Mf 14:15; 2Mf 17:18; Sl 52:5; Lu 21:24
Deut. 29:28Eza 9:7; Da 9:7
Deut. 29:29Yes 55:8; Aro 11:33; 1Ak 2:16
Deut. 29:29Amo 3:7; Mt 11:27; Aef 3:5
Deut. 29:29Sl 78:5; Mla 12:13; 1Yo 5:3
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
  • 18
  • 19
  • 20
  • 21
  • 22
  • 23
  • 24
  • 25
  • 26
  • 27
  • 28
  • 29
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Deuteronomo 29:1-29

Deuteronomo

29 Awa ndi mawu a pangano limene Yehova analamula Mose kuti achite ndi ana a Isiraeli m’dziko la Mowabu, kuwonjezera pa pangano limene anachita nawo ku Horebe.+

2 Choncho Mose anaitana Aisiraeli onse ndi kuwauza kuti: “Inuyo ndinu amene munaona ndi maso m’dziko la Iguputo zonse zimene Yehova anachitira Farao, atumiki ake onse ndi dziko lake lonse.+ 3 Inuyo munaona mayesero,+ zizindikiro zazikulu+ zija ndi zozizwitsa.+ 4 Koma Yehova sanakupatseni mtima woti muthe kuzindikira, maso oti muthe kuona ndi makutu oti muthe kumva, kufikira lero.+ 5 ‘Pamene ndinali kukutsogolerani kwa zaka 40 m’chipululu,+ zovala zanu sizinathe ndiponso nsapato zanu sizinathe kumapazi anu.+ 6 Simunadye mkate,+ simunamwe vinyo ndi zakumwa zina zoledzeretsa, kuti mudziwe kuti ine ndine Yehova Mulungu wanu.’ 7 Ndiyeno munafika pamalo ano, ndipo Sihoni mfumu ya Hesiboni+ ndi Ogi+ mfumu ya Basana anatuluka kudzamenyana nafe nkhondo, koma tinawagonjetsa.+ 8 Kenako tinatenga dziko lawo ndi kulipereka monga cholowa kwa fuko la Rubeni, fuko la Gadi ndi hafu ya fuko la Manase.+ 9 Choncho muzisunga mawu a pangano ili kuti zonse zimene muzichita zizikuyenderani bwino.+

10 “Nonsenu mwaima pano lero pamaso pa Yehova Mulungu wanu, inu atsogoleri a mafuko, akulu anu, atsogoleri anu, mwamuna aliyense wa mu Isiraeli,+ 11 ana anu, akazi anu,+ alendo+ okhala mkati mwa msasa wanu, kuyambira wokutolerani nkhuni mpaka wokutungirani madzi,+ 12 kuti muchite pangano+ ndi Yehova Mulungu wanu mwa kulumbira, pangano limene Yehova Mulungu wanu akuchita nanu lero.+ 13 Cholinga chake n’chakuti akukhazikitseni lero monga anthu ake+ ndi kuti akuonetseni kuti ndi Mulungu wanu,+ monga mmene anakulonjezerani ndiponso monga mmene analumbirira makolo anu, Abulahamu,+ Isaki+ ndi Yakobo.+

14 “Tsopano sindikuchita pangano ili mwa lumbiro ndi inu nokha ayi,+ 15 koma ndikuchita pangano ili ndi anthu amene aimirira ndi ife pano lero pamaso pa Yehova Mulungu wanu, komanso ndi awo amene sitili nawo pano lero.+ 16 (Pakuti inu mukudziwa bwino mmene tinali kukhalira m’dziko la Iguputo ndi mmene tinadutsira pakati pa anthu a mitundu ina. Podutsa pakati pa mitundu imeneyo,+ 17 munaona zinthu zawo zonyansa ndi mafano awo onyansa,*+ mafano amtengo ndi amwala, asiliva ndi agolide amene anali nawo.) 18 Cholinga cha pangano limeneli n’chakuti, pakati panu pasapezeke mwamuna, mkazi, banja kapena fuko limene mtima wake ukupatuka kusiyana ndi Yehova Mulungu wathu, ndi kupita kukatumikira milungu ya mitundu inayo,+ kuti pakati panu pasapezeke muzu wotulutsa chomera chakupha ndi chitsamba chowawa.+

19 “Ndiyeno zikachitika kuti wina amene wamva mawu a lumbiro+ ili, walankhula modzitama mumtima mwake kuti, ‘Ndidzakhala ndi mtendere+ ngakhale kuti ndidzayenda motsatira zofuna za mtima wanga,’+ koma ali ndi cholinga chowononga wina aliyense, mofanana ndi kukokolola mtengo wothiriridwa bwino ndi wosathiriridwa womwe, 20 Yehova sadzafuna kukhululukira+ munthu woteroyo, m’malomwake mkwiyo+ ndi ukali+ wa Yehova udzamuyakira,+ ndipo matemberero onse olembedwa m’buku+ ili adzakhala pa iye, motero Yehova adzafafanizadi dzina la munthuyo pansi pa thambo. 21 Choncho Yehova adzam’patula+ pa mafuko onse a Isiraeli kuti amudzetsere tsoka, mogwirizana ndi matemberero onse a pangano lolembedwa m’buku ili la chilamulo.

22 “Pamenepo m’badwo wa m’tsogolo, ana anu amene adzabwera pambuyo panu, ndiponso mlendo amene adzachokera kudziko lakutali, akadzaona miliri ndi nthenda zimene Yehova wakantha nazo dzikolo,+ adzanena mawu. 23 Adzanena mawuwo akadzaonanso sulufule, mchere+ ndi kutentha,+ moti m’dzikomo simungabzalidwe mbewu, simungaphuke kalikonse ndipo simungamere chomera chilichonse, mofanana ndi Sodomu ndi Gomora,+ Adima+ ndi Zeboyimu,+ mizinda imene Yehova anaiwononga mu ukali ndi mkwiyo wake.+ 24 Mitundu yonse idzanena kuti, ‘N’chifukwa chiyani Yehova wachitira dzikoli zimenezi?+ N’chifukwa chiyani mkwiyo wake wayaka kwambiri chonchi?’ 25 Pamenepo anthu adzanena kuti, ‘N’chifukwa chakuti anataya pangano+ la Yehova Mulungu wa makolo awo, limene anapangana nawo pamene anali kuwatulutsa m’dziko la Iguputo.+ 26 Ndipo anapita kukatumikira milungu ina ndi kuigwadira, milungu imene sanaidziwe, imenenso sanaloledwe kuti aziilambira.+ 27 Pamenepo mkwiyo wa Yehova unayakira dziko limeneli mwa kulibweretsera matemberero onse olembedwa m’buku ili.+ 28 Choncho Yehova anawazula m’dziko lawo atapsa mtima,+ ali ndi ukali ndiponso mkwiyo waukulu n’kuwataya m’dziko lina monga mmene zilili lero.’+

29 “Zinthu zobisika+ ndi za Yehova Mulungu wathu, koma zinthu zoululidwa+ ndi zathu ndi ana athu mpaka kalekale, kuti titsatire mawu onse a chilamulo ichi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena