Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nyimbo ya Solomo 4
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Nyimbo ya Solomo 4:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 45:11
  • +Nym 1:15
  • +Ge 24:65
  • +Nym 6:5
  • +Nu 32:1; De 3:12

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    11/15/2006, tsa. 19

Nyimbo ya Solomo 4:2

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nym 6:6

Nyimbo ya Solomo 4:3

Mawu a M'munsi

  • *

    “Khangaza” ndi mtundu wa chipatso. Ena amati chimanga chachizungu, mwina chifukwa choti njere zake zimaoneka ngati chimanga.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 37:30; 45:2
  • +Nym 6:7

Nyimbo ya Solomo 4:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nym 1:10
  • +Ne 3:25; Nym 7:4
  • +2Sa 8:7; 2Mf 11:10; Eze 27:11

Nyimbo ya Solomo 4:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nym 7:3
  • +Nym 2:16

Nyimbo ya Solomo 4:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nym 2:17
  • +Mla 2:5

Nyimbo ya Solomo 4:7

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nym 4:1
  • +2Ak 11:2; Aef 1:4; 2Pe 3:14

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    1/15/2015, tsa. 30

    11/15/2006, tsa. 20

    Galamukani!,

    5/8/1989, tsa. 14

Nyimbo ya Solomo 4:8

Mawu a M'munsi

  • *

    Ena amati “anyalugwe.”

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yoh 3:29; Chv 21:9
  • +De 3:25
  • +De 3:9
  • +Sl 133:3

Nyimbo ya Solomo 4:9

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nym 5:1
  • +Sl 45:14; Chv 19:7
  • +Miy 5:19

Nyimbo ya Solomo 4:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nym 1:2; 7:12
  • +Est 2:12; Nym 1:3, 12

Nyimbo ya Solomo 4:11

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Miy 16:24
  • +Miy 24:13; Nym 5:1
  • +Sl 45:8

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    1/15/2015, tsa. 30

    11/15/2006, tsa. 19

Nyimbo ya Solomo 4:12

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nym 6:2

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    1/15/2015, tsa. 32

    11/15/2006, tsa. 20

    11/1/2000, ptsa. 11-12

    11/15/1987, tsa. 25

Nyimbo ya Solomo 4:13

Mawu a M'munsi

  • *

    Mawu ake enieni, “paradaiso.”

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nym 7:13
  • +Nym 1:12; Yoh 12:3

Nyimbo ya Solomo 4:14

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nym 2:1
  • +Eks 30:23; Yes 43:24
  • +Miy 7:17; Chv 18:13
  • +Nu 24:6; Sl 45:8
  • +Eks 30:34; Eze 27:22; 2Ak 2:14

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    2/1/2014, tsa. 10

Nyimbo ya Solomo 4:15

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 26:19
  • +Yer 18:14

Nyimbo ya Solomo 4:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mla 1:6
  • +Nym 5:1

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Nyimbo 4:1Sl 45:11
Nyimbo 4:1Nym 1:15
Nyimbo 4:1Ge 24:65
Nyimbo 4:1Nym 6:5
Nyimbo 4:1Nu 32:1; De 3:12
Nyimbo 4:2Nym 6:6
Nyimbo 4:3Sl 37:30; 45:2
Nyimbo 4:3Nym 6:7
Nyimbo 4:4Nym 1:10
Nyimbo 4:4Ne 3:25; Nym 7:4
Nyimbo 4:42Sa 8:7; 2Mf 11:10; Eze 27:11
Nyimbo 4:5Nym 7:3
Nyimbo 4:5Nym 2:16
Nyimbo 4:6Nym 2:17
Nyimbo 4:6Mla 2:5
Nyimbo 4:7Nym 4:1
Nyimbo 4:72Ak 11:2; Aef 1:4; 2Pe 3:14
Nyimbo 4:8Yoh 3:29; Chv 21:9
Nyimbo 4:8De 3:25
Nyimbo 4:8De 3:9
Nyimbo 4:8Sl 133:3
Nyimbo 4:9Nym 5:1
Nyimbo 4:9Sl 45:14; Chv 19:7
Nyimbo 4:9Miy 5:19
Nyimbo 4:10Nym 1:2; 7:12
Nyimbo 4:10Est 2:12; Nym 1:3, 12
Nyimbo 4:11Miy 16:24
Nyimbo 4:11Miy 24:13; Nym 5:1
Nyimbo 4:11Sl 45:8
Nyimbo 4:12Nym 6:2
Nyimbo 4:13Nym 7:13
Nyimbo 4:13Nym 1:12; Yoh 12:3
Nyimbo 4:14Nym 2:1
Nyimbo 4:14Eks 30:23; Yes 43:24
Nyimbo 4:14Miy 7:17; Chv 18:13
Nyimbo 4:14Nu 24:6; Sl 45:8
Nyimbo 4:14Eks 30:34; Eze 27:22; 2Ak 2:14
Nyimbo 4:15Ge 26:19
Nyimbo 4:15Yer 18:14
Nyimbo 4:16Mla 1:6
Nyimbo 4:16Nym 5:1
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Nyimbo ya Solomo 4:1-16

Nyimbo ya Solomo

4 “Ndiwe wokongola kwabasi,+ wokondedwa wanga. Ndiwe chiphadzuwa. Maso ako ali ngati maso a njiwa+ munsalu yako yophimba kumutuyo.+ Tsitsi lako likuoneka ngati gulu la mbuzi+ zimene zikudumphadumpha potsetsereka kuchokera kudera lamapiri la Giliyadi.+ 2 Mano ako ali ngati gulu la nkhosa zazikazi zomwe angozimeta kumene,+ zimene zikuchokera kozisambitsa, zonse zitabereka mapasa, popanda imene ana ake afa. 3 Milomo yako ili ngati chingwe chofiira kwambiri, ndipo kulankhula kwako n’kosangalatsa.+ M’mbali mwa mutu wako muli ngati khangaza* logamphula pakati, munsalu yako yophimba kumutuyo.+ 4 Khosi lako+ lili ngati nsanja+ ya Davide. Lili ngati nsanja yomangidwa ndi miyala yokhala m’mizeremizere, yomwe akolekapo zishango 1,000, zishango zonse zozungulira+ za amuna amphamvu. 5 Mabere ako awiri+ ali ngati ana awiri aang’ono, ngati ana amapasa a insa yaikazi, amene akudya msipu pakati pa maluwa akutchire.”+

6 “Nthawi ya kamphepo kayaziyazi isanakwane+ ndiponso mithunzi isanachoke, ndipita kuphiri la mule ndiponso kuphiri la lubani.”+

7 “Ndiwe wokongola paliponse,+ wokondedwa wanga, ndipo mwa iwe mulibe chilema chilichonse.+ 8 Tiye tichokere limodzi ku Lebanoni, iwe mkwatibwi wanga,+ tiye tichoke ku Lebanoni.+ Utsetsereke kuchokera pamwamba pa phiri la Amana, kuchokera pamwamba pa phiri la Seniri,+ ngakhalenso pamwamba pa phiri la Herimoni.+ Utsetsereke kuchokera m’mapanga a mikango, ndiponso kuchokera kumapiri a akambuku.* 9 Wachititsa mtima wanga kugunda, iwe mlongo wanga,+ mkwatibwi wanga.+ Wachititsa mtima wanga kugunda ndi diso lako limodzi lokha,+ ndiponso ndi diso limodzi lokha la mkanda wa m’khosi mwako. 10 Chikondi chimene umandisonyeza n’chokoma,+ iwe mlongo wanga, mkwatibwi wanga. Chikondi chimene umandisonyeza n’chabwino kuposa vinyo ndipo kununkhira kwa mafuta ako odzola n’koposa zonunkhira za mitundu yonse.+ 11 Milomo yako imangokhalira kukha uchi wapachisa,+ iwe mkwatibwi wanga. Uchi+ ndi mkaka zili kuseri kwa lilime lako, ndipo kununkhira kwa zovala zako kuli ngati kununkhira+ kwa nkhalango ya Lebanoni. 12 Mlongo wanga, mkwatibwi wanga, ali ngati munda wotchingidwa ndi mpanda.+ Iye ali ngati munda wotchingidwa ndi mpanda, ndiponso ngati kasupe wotsekedwa. 13 Khungu lako lili ngati munda wokongola* wokhala ndi mitengo ya makangaza ya zipatso zabwino kwambiri,+ mitengo ya maluwa ofiirira, mitengo ya nado,+ 14 maluwa a safironi,+ mabango onunkhira,+ sinamoni,+ komanso mitengo yosiyanasiyana ya lubani, mule, aloye,+ ndi zonunkhira zonse zabwino kwambiri.+ 15 Khungu lako lilinso ngati kasupe wa m’munda, chitsime cha madzi abwino,+ ndiponso timitsinje tochokera ku Lebanoni.+ 16 Dzuka, iwe mphepo yakumpoto. Bwera, iwe mphepo yakum’mwera.+ Womba pamunda wanga+ kuti kununkhira kwake kumveke.”

“Wachikondi wanga alowe m’munda wake kuti adzadye zipatso zake zokoma kwambiri.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena