Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 6
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Deuteronomo 6:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 4:1, 10

Deuteronomo 6:2

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 20:20; Yos 24:14; Yob 28:28; Sl 111:10; 128:1
  • +Ge 18:19; De 4:9
  • +De 5:16; Miy 3:2

Deuteronomo 6:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 5:32; 2Mf 21:8
  • +Mla 8:12; Yes 3:10
  • +Ge 13:16

Deuteronomo 6:4

Mawu a M'munsi

  • *

    Kapena kuti “Yehova ndi Mulungu wathu, Yehova ndi mmodzi [kapena, pali Yehova mmodzi].”

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 5:7; Yes 42:8; Zek 14:9; Mko 12:29; 1Ak 8:6

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    6/2016, ptsa. 18-22

    Nsanja ya Olonda,

    3/1/2012, tsa. 23

    12/15/1992, tsa. 29

    Kukambitsirana, ptsa. 392, 402

Deuteronomo 6:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 10:12; Mt 22:37
  • +De 11:13; 30:6
  • +Mko 12:30; Lu 10:27

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    5/15/2007, ptsa. 15-16

    6/15/2005, tsa. 20

    10/1/1995, tsa. 13

Deuteronomo 6:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 11:18; Miy 7:3

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale, lesson 50

    Nsanja ya Olonda,

    4/1/2008, tsa. 14

    5/15/2007, ptsa. 15-16

    4/1/2006, ptsa. 8-9

    6/15/2005, tsa. 20

    4/1/2005, ptsa. 11-12

    6/1/1998, tsa. 20

    12/1/1996, tsa. 11

    7/1/1991, tsa. 26

    8/15/1988, tsa. 11

    Chinsinsi cha Banja, ptsa. 55-57, 58-59, 70-71

Deuteronomo 6:7

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 18:19; De 4:9; 11:19; Miy 22:6; Aef 6:4
  • +Miy 6:22

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale, lesson 50

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    12/2019, tsa. 26

    Nsanja ya Olonda,

    8/15/2013, tsa. 16

    4/1/2008, tsa. 14

    9/1/2007, tsa. 22

    5/15/2007, ptsa. 15-16

    11/1/2006, ptsa. 4-6

    4/1/2006, ptsa. 8-9

    6/15/2005, ptsa. 20-21

    4/15/2005, ptsa. 6-7

    4/1/2005, ptsa. 11-12

    1/1/2005, tsa. 26

    6/15/2004, tsa. 5

    6/1/1998, ptsa. 20-22

    12/1/1996, tsa. 11

    5/1/1995, tsa. 10

    6/15/1989, tsa. 20

    Chinsinsi cha Banja, ptsa. 55-57, 58-59, 70-71

Deuteronomo 6:8

Mawu a M'munsi

  • *

    Mawu ake enieni, “pakati pa maso ako.”

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Miy 3:3; 7:3
  • +Eks 13:9, 16; De 11:18

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    4/1/2005, tsa. 13

    9/15/2004, tsa. 26

    7/15/1995, tsa. 29

    5/1/1995, ptsa. 11-12

    8/15/1988, tsa. 11

Deuteronomo 6:9

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 11:20

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    4/1/2005, tsa. 13

    7/15/1995, tsa. 29

    5/1/1995, ptsa. 11-12

Deuteronomo 6:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 15:18
  • +Yos 24:13; Sl 105:44

Deuteronomo 6:11

Mawu a M'munsi

  • *

    Onani Matanthauzo a Mawu Ena.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 8:10

Deuteronomo 6:12

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Owe 3:7; Yer 2:32

Deuteronomo 6:13

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 10:12; 13:4; Sl 34:9; 128:1
  • +Lu 4:8
  • +De 10:20; Owe 21:7; Yer 12:16

Deuteronomo 6:14

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 34:14; De 8:19; Yer 25:6

Deuteronomo 6:15

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 20:5; De 4:24; Yos 24:19; Nah 1:2
  • +Eks 32:10; Nu 25:3; De 11:17; Owe 2:14
  • +1Mf 13:34; 2Mf 17:18

Deuteronomo 6:16

Mawu a M'munsi

  • *

    Dzina lakuti “Masa” limatanthauza “Kuyesa; Mayesero.”

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mt 4:7; Lu 4:12; 1Ak 10:9
  • +Eks 17:2; De 33:8; Sl 95:8; Ahe 3:8

Deuteronomo 6:17

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 11:13; Eze 20:11
  • +1Mf 2:3
  • +De 4:1; Ne 9:13
  • +De 11:22; Sl 119:4

Deuteronomo 6:18

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 5:33
  • +Ge 15:18

Deuteronomo 6:19

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 23:30; Nu 33:52

Deuteronomo 6:20

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 13:14

Deuteronomo 6:21

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 15:6

Deuteronomo 6:22

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 7:3; De 7:19
  • +De 4:34

Deuteronomo 6:23

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 13:5; De 1:8

Deuteronomo 6:24

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 5:1; 1Mf 2:3
  • +De 10:12; Sl 111:10; Miy 14:27; Mla 8:12
  • +De 4:1; Lu 10:28; Aga 3:12

Deuteronomo 6:25

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 18:5; Mla 12:13
  • +Aro 10:5

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Deut. 6:1De 4:1, 10
Deut. 6:2Eks 20:20; Yos 24:14; Yob 28:28; Sl 111:10; 128:1
Deut. 6:2Ge 18:19; De 4:9
Deut. 6:2De 5:16; Miy 3:2
Deut. 6:3De 5:32; 2Mf 21:8
Deut. 6:3Mla 8:12; Yes 3:10
Deut. 6:3Ge 13:16
Deut. 6:4De 5:7; Yes 42:8; Zek 14:9; Mko 12:29; 1Ak 8:6
Deut. 6:5De 10:12; Mt 22:37
Deut. 6:5De 11:13; 30:6
Deut. 6:5Mko 12:30; Lu 10:27
Deut. 6:6De 11:18; Miy 7:3
Deut. 6:7Ge 18:19; De 4:9; 11:19; Miy 22:6; Aef 6:4
Deut. 6:7Miy 6:22
Deut. 6:8Miy 3:3; 7:3
Deut. 6:8Eks 13:9, 16; De 11:18
Deut. 6:9De 11:20
Deut. 6:10Ge 15:18
Deut. 6:10Yos 24:13; Sl 105:44
Deut. 6:11De 8:10
Deut. 6:12Owe 3:7; Yer 2:32
Deut. 6:13De 10:12; 13:4; Sl 34:9; 128:1
Deut. 6:13Lu 4:8
Deut. 6:13De 10:20; Owe 21:7; Yer 12:16
Deut. 6:14Eks 34:14; De 8:19; Yer 25:6
Deut. 6:15Eks 20:5; De 4:24; Yos 24:19; Nah 1:2
Deut. 6:15Eks 32:10; Nu 25:3; De 11:17; Owe 2:14
Deut. 6:151Mf 13:34; 2Mf 17:18
Deut. 6:16Mt 4:7; Lu 4:12; 1Ak 10:9
Deut. 6:16Eks 17:2; De 33:8; Sl 95:8; Ahe 3:8
Deut. 6:17De 11:13; Eze 20:11
Deut. 6:171Mf 2:3
Deut. 6:17De 4:1; Ne 9:13
Deut. 6:17De 11:22; Sl 119:4
Deut. 6:18De 5:33
Deut. 6:18Ge 15:18
Deut. 6:19Eks 23:30; Nu 33:52
Deut. 6:20Eks 13:14
Deut. 6:21Eks 15:6
Deut. 6:22Eks 7:3; De 7:19
Deut. 6:22De 4:34
Deut. 6:23Eks 13:5; De 1:8
Deut. 6:24De 5:1; 1Mf 2:3
Deut. 6:24De 10:12; Sl 111:10; Miy 14:27; Mla 8:12
Deut. 6:24De 4:1; Lu 10:28; Aga 3:12
Deut. 6:25Le 18:5; Mla 12:13
Deut. 6:25Aro 10:5
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
  • 18
  • 19
  • 20
  • 21
  • 22
  • 23
  • 24
  • 25
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Deuteronomo 6:1-25

Deuteronomo

6 “Tsopano amenewa ndiwo malamulo, malangizo ndi zigamulo zimene Yehova Mulungu wanu walamula kuti ndikuphunzitseni,+ kuti muzikazitsatira m’dziko limene mukuwolokerako kukalitenga kukhala lanu. 2 Muyenera kuphunzira zimenezi kuti muziopa+ Yehova Mulungu wanu, n’cholinga choti masiku onse a moyo wanu muzisunga mfundo zake ndi malamulo ake amene ndikukuuzani, inuyo, ana anu ndi zidzukulu zanu,+ ndiponso kuti masiku anu atalike.+ 3 Ndipo inu Aisiraeli, muzimvetsera ndi kutsatira mfundo ndi malamulo ake mosamala,+ kuti zinthu zikuyendereni bwino,+ ndi kuti muchuluke kwambiri m’dziko loyenda mkaka ndi uchi, monga mmene Yehova Mulungu wa makolo anu anakulonjezerani.+

4 “Tamverani, Aisiraeli inu: Yehova Mulungu wathu ndi Yehova mmodzi.*+ 5 Uzikonda Yehova Mulungu wako ndi mtima wako wonse,+ moyo wako wonse,+ ndi mphamvu zako zonse.+ 6 Ndipo mawu awa amene ndikukulamula lero azikhala pamtima pako,+ 7 ndi kuwakhomereza mwa ana ako.+ Uzilankhula nawo za mawuwo ukakhala pansi m’nyumba mwako, poyenda pamsewu, pogona+ ndi podzuka. 8 Uziwamanga padzanja lako+ monga chizindikiro, ndipo azikhala ngati chomanga pamphumi pako,*+ 9 ndiponso uziwalemba pafelemu la khomo la nyumba yako ndi pazipata za mzinda wanu.+

10 “Ndiyeno Yehova Mulungu wako akadzakulowetsa m’dziko limene analumbirira makolo ako Abulahamu, Isaki ndi Yakobo kuti adzakupatsa,+ dziko lokhala ndi mizinda ikuluikulu yooneka bwino imene sunamange ndiwe,+ 11 yokhalanso ndi nyumba zodzaza ndi zinthu zonse zabwino zimene sunaikemo ndiwe, ndi zitsime* zimene sunakumbe ndiwe, minda ya mpesa ndi mitengo ya maolivi imene sunabzale ndiwe, n’kudya ndi kukhuta,+ 12 samala kuti usaiwale+ Yehova amene anakutulutsa m’dziko la Iguputo, m’nyumba yaukapolo. 13 Uziopa Yehova Mulungu wako+ ndi kum’tumikira,+ ndipo uzilumbira pa dzina lake.+ 14 Musatsatire milungu ina, milungu iliyonse ya anthu okuzungulirani,+ 15 (pakuti Yehova Mulungu wanu amene ali pakati panu ndi Mulungu wofuna kuti anthu azidzipereka kwa iye yekha basi).+ Musatsatire milungu ina kuopera kuti mkwiyo wa Yehova Mulungu wanu ungakuyakireni,+ ndipo angakufafanizeni padziko lapansi.+

16 “Musamuyese, Yehova Mulungu wanu,+ mmene munamuyesera pa Masa.*+ 17 Muzionetsetsa kuti mukusunga malamulo a Yehova Mulungu wanu,+ maumboni ake+ ndi zigamulo+ zake zimene wakupatsani.+ 18 Ndipo muzichita zoyenera ndi zabwino pamaso pa Yehova kuti zikuyendereni bwino,+ ndi kuti mukalowedi m’dziko labwino limene Yehova analumbirira makolo anu,+ ndi kulitenga kukhala lanu, 19 mwa kukankhira adani anu kutali monga mmene Yehova analonjezera.+

20 “Mwana wako akadzakufunsa tsiku lina m’tsogolo+ kuti, ‘Kodi zikumbutso, malangizo ndi zigamulo izi zimene Yehova Mulungu wathu anakupatsani, zimatanthauza chiyani?’ 21 Pamenepo mwana wakoyo udzamuyankhe kuti, ‘Tinakhala akapolo a Farao ku Iguputo, koma Yehova anatitulutsa ku Iguputoko ndi dzanja lamphamvu.+ 22 Motero Yehova anali kuchita zizindikiro ndi zozizwitsa+ zazikulu ndiponso zodzetsa masoka, mu Iguputo yense, kwa Farao ndi kwa onse a m’nyumba mwake ife tikuona.+ 23 Ndipo anatitulutsa kumeneko kuti atibweretse kuno kudzatipatsa dziko limene analumbirira makolo athu.+ 24 Choncho Yehova anatilamula kuti tizitsatira malangizo onsewa,+ tiziopa Yehova Mulungu wathu ndi kupindula nthawi zonse,+ kuti tikhale ndi moyo monga mmene zilili lero.+ 25 Ndipo tikatsatira malamulo onsewa monga mmene Yehova Mulungu wathu watilamulira,+ ndiye kuti tikuchita chilungamo+ pamaso pake.’

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena