Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 20
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Deuteronomo 20:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yos 11:4
  • +Eks 13:3; De 3:22; 31:6; Sl 20:7; 46:7; Miy 21:31; Aro 8:31

Deuteronomo 20:2

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 31:6; Owe 20:28; 1Sa 30:7; 2Mb 13:12

Deuteronomo 20:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 27:3; Yes 35:4; 41:10
  • +Sl 3:6

Deuteronomo 20:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 14:14; De 32:30; Yos 23:10

Deuteronomo 20:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 31:14; De 16:18
  • +Mla 2:24

Deuteronomo 20:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 145:9; Mla 3:13

Deuteronomo 20:7

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 24:5

Deuteronomo 20:8

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Owe 7:3
  • +Nu 13:33; 14:1; 32:9; De 1:28; Mac 21:13

Deuteronomo 20:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yos 11:19

Deuteronomo 20:11

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 25:46; De 20:15; Yos 9:22, 27

Deuteronomo 20:12

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 120:7

Deuteronomo 20:13

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 31:7

Deuteronomo 20:14

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 31:9, 18
  • +Yos 8:2
  • +Nu 31:12, 27; 2Mb 14:13; Sl 68:12
  • +Yos 22:8

Deuteronomo 20:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yos 6:17; 10:28; 11:11

Deuteronomo 20:17

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 7:1

Deuteronomo 20:18

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 34:15; De 7:4; Yos 23:12; Sl 106:35; Yes 2:6; 1Ak 5:6; 15:33

Deuteronomo 20:19

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ne 9:25

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Yandikirani, tsa. 135

Deuteronomo 20:20

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Mb 26:15; Mla 9:14; Yes 37:33; Yer 6:6; Eze 17:17

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Deut. 20:1Yos 11:4
Deut. 20:1Eks 13:3; De 3:22; 31:6; Sl 20:7; 46:7; Miy 21:31; Aro 8:31
Deut. 20:2Nu 31:6; Owe 20:28; 1Sa 30:7; 2Mb 13:12
Deut. 20:3Sl 27:3; Yes 35:4; 41:10
Deut. 20:3Sl 3:6
Deut. 20:4Eks 14:14; De 32:30; Yos 23:10
Deut. 20:5Nu 31:14; De 16:18
Deut. 20:5Mla 2:24
Deut. 20:6Sl 145:9; Mla 3:13
Deut. 20:7De 24:5
Deut. 20:8Owe 7:3
Deut. 20:8Nu 13:33; 14:1; 32:9; De 1:28; Mac 21:13
Deut. 20:10Yos 11:19
Deut. 20:11Le 25:46; De 20:15; Yos 9:22, 27
Deut. 20:12Sl 120:7
Deut. 20:13Nu 31:7
Deut. 20:14Nu 31:9, 18
Deut. 20:14Yos 8:2
Deut. 20:14Nu 31:12, 27; 2Mb 14:13; Sl 68:12
Deut. 20:14Yos 22:8
Deut. 20:16Yos 6:17; 10:28; 11:11
Deut. 20:17De 7:1
Deut. 20:18Eks 34:15; De 7:4; Yos 23:12; Sl 106:35; Yes 2:6; 1Ak 5:6; 15:33
Deut. 20:19Ne 9:25
Deut. 20:202Mb 26:15; Mla 9:14; Yes 37:33; Yer 6:6; Eze 17:17
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
  • 18
  • 19
  • 20
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Deuteronomo 20:1-20

Deuteronomo

20 “Mukapita kunkhondo kukamenyana ndi adani anu, musachite nawo mantha mukaona kuti ali ndi mahatchi ndi magaleta ankhondo,+ ndiponso mukaona kuti adani anuwo ndi ochuluka kwambiri kuposa inu. Yehova Mulungu wanu, amene anakutulutsani m’dziko la Iguputo ali ndi inu.+ 2 Mukayandikira kuti mumenyane nawo, wansembe azifika pafupi nanu ndi kulankhula ndi anthu+ 3 kuti, ‘Mverani Aisiraeli inu. Lero mukuyandikira adani anu kuti mumenyane nawo. Mitima yanu isachite mantha.+ Musaope ndipo musathawe mwamantha kapena kunjenjemera chifukwa cha iwo,+ 4 chifukwa Yehova Mulungu wanu akuyenda limodzi nanu kuti akumenyereni nkhondo ndi kukupulumutsani kwa adani anu.’+

5 “Atsogoleri+ nawonso azilankhula ndi anthuwo kuti, ‘Kodi pali amene wamanga nyumba yatsopano koma sanaitsegulire? Achoke ndi kubwerera kunyumba yakeyo, kuopera kuti angafe pankhondo, ndipo munthu wina angatsegulire nyumbayo.+ 6 Kodi pali amene walima munda wa mpesa koma sanayambe kukolola zipatso zake? Achoke ndi kubwerera kunyumba yake, kuopera kuti angafe pankhondo ndipo munthu wina angakolole za m’munda wakewo.+ 7 Kodi pali amene analonjeza mkazi kuti adzamukwatira ndipo sanamutenge? Achoke ndi kubwerera kunyumba yake,+ kuopera kuti angafe pankhondo ndipo mwamuna wina angatenge mkaziyo.’ 8 Ndiyeno atsogoleri apitirize kulankhula ndi anthuwo kuti, ‘Kodi pali wamantha ndi wosalimba mtima?+ Achoke ndi kubwerera kunyumba yake, kuti angachititse mantha mitima ya abale ake ngati mmene wachitira mtima wake.’+ 9 Atsogoleriwo akamaliza kulankhula ndi anthu, azisankha akulu a magulu ankhondo oti akhale patsogolo pa anthuwo.

10 “Mukayandikira mzinda kuti mumenyane nawo, muzilengeza kumzindawo mfundo za mtendere.+ 11 Ndiyeno ngati mzindawo wakupatsani yankho la mtendere ndipo akutsegulirani zipata zake, pamenepo anthu onse opezeka mmenemo azikhala anu kuti azikugwirirani ntchito yaukapolo. Iwo azikutumikirani.+ 12 Koma ngati mzindawo sukukhazikitsa mtendere ndi inu,+ ndipo ukuchita nanu nkhondo, moti inuyo mwauzungulira, 13 Yehova Mulungu wanu adzaupereka ndithu m’manja mwanu, ndipo zikatero muzipha mwamuna aliyense ndi lupanga.+ 14 Koma musaphe akazi, ana aang’ono,+ ziweto+ ndi chilichonse chopezeka mumzindawo. Muzifunkha+ zinthu zonse za mumzindawo ndipo muzidya zimene mwafunkha kwa adani anu amene Yehova Mulungu wanu wakupatsani.+

15 “Muzichita zimenezi ndi mizinda yonse yakutali kwambiri ndi inu imene siili pakati pa mizinda ya mitundu iyi. 16 Mizinda yokhayi ya anthu awa a mitundu ina imene Yehova Mulungu wanu akukupatsani monga cholowa, ndi imene simuyenera kusiyamo chilichonse chopuma chili chamoyo,+ 17 chifukwa muyenera kuwawononga ndithu. Mukawononge Ahiti, Aamori, Akanani, Aperezi, Ahivi ndi Ayebusi,+ monga mmene Yehova Mulungu wanu anakulamulirani. 18 Mukawawononge kuti asakakuphunzitseni kuchita zinthu zawo zonse zonyansa zimene achitira milungu yawo, kuti mungachimwire Yehova Mulungu wanu.+

19 “Mukazungulira mzinda kwa masiku ambiri mwa kumenyana nawo kuti muulande, musawononge mitengo yake mwa kuisamulira nkhwangwa. Muyenera kudya zipatso za mitengoyo, chotero simuyenera kuidula.+ Kodi mtengo wa m’munda ndi munthu kuti muwuukire? 20 Mungathe kuwononga mtengo wokhawo umene mukuudziwa kuti subereka zipatso zakudya. Mtengo woterowo mungaudule ndi kumangira mpanda wozungulira+ mzinda wa adani umene ukuchita nanu nkhondo, kufikira mzindawo utagwa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena